score
float32
1.04
1.25
Chichewa
stringlengths
10
497
Tigrinya
stringlengths
10
498
1.197575
"[Mulungu] adzapukuta misozi yonse m'maso mwawo."
ኣምላኽ እውን ካብ ኣዒንቶም ንብዓት ዘበለ ኺደርዝ እዩ" ትብል።
1.197515
3 Wodala iye amene awerenga, ndi iwo amene akumva mawu a chinenerocho, nasunga zolembedwa momwemo: pakuti nthawi yayandikira.
3እቲ እዙይ ዝፍጸመሉ ዘመን ቀረባ ስለ ዝኾነ ድማ እቲ ነዝ ቓል ትንቢት እዙይ ዘንብብ ብፁዕ እዩ፤ እቶም ዝሰምዕዎን ነቲ ኣብኡ ተጽሒፉ ዘሎ ዝፍጽምዎንውን ብፁዓን እዮም።
1.197395
Mwamutopetsa ponena kuti, "Aliyense amene amachita zoyipa ndi wabwino pamaso pa Yehova ndipo iye amakondwera naye" kapena pofunsa kuti, "Ali kuti Mulungu woweruza mwachilungamo?"
'ክፉእ ዚገብር ዘበለ ኣብ ቅድሚ ኣዒንቲ የሆዋ ጽቡቕ እዩ፣ ንሱ እውን ብእኡ ባህ ይብሎ እዩ' ብምባልኩም+ ወይ 'ፍትሒ ኣምላኽ ኣበይ ኣሎ፧' ብምባልኩም እዩ።
1.197115
10 Timakhala pa ubwenzi ndi Yehova.
10 ምስ ኣምላኽ ሰላማዊ ርክብ ይህልወና።
1.197085
12 Luso ndi mphamvu zathu.
12 ጕልበትናን ክእለትናን።
1.197059
Komabe alipo ena mwa inu amene sakukhulupirira."
ገለ ኻባኻትኩም ግና ዘይኣምኑ ኣለዉ" በሎም።
1.196903
Koma ngati inu simutembenuka mtima, inunso mudzawonongeka nonse.
5ኣይፋሉን፤ እንተ ዘይተነሲሕኹምስ ኲልኻትኩምውን ከምኣቶም ክትጠፍኡ ኢኹም በሎም።
1.196789
Koma ngati inu simutembenuka mtima, inunso mudzawonongeka nonse."
5ኣይፋሉን፤ እንተ ዘይተነሲሕኹምስ ኲልኻትኩምውን ከምኣቶም ክትጠፍኡ ኢኹም በሎም።
1.196577
Mneneriyo ndi amene anali "mbewu" yolonjezedwa ija.
እቲ ነብዪ እቲ ኸኣ፡ እቲ መብጽዓ እተኣትወሉ "ዘርኢ" እዩ።
1.196553
Ngati timakonda Mulungu, kodi tiziona bwanji misonkhano?
ንኣምላኽ ነፍቅሮ እንተ ዄንና፡ ንኣኼባታትና ብኸመይ ኢና እንርእዮ፧
1.196525
ndipo ndidzayenda mʼchoonadi chanu;
ብሓቅኻ ኽመላለስ እየ።
1.196522
Ngakhale bambo anga akudziwa zimenezi.'
ኣቦይ እውን ነዚ ይፈልጦ እዩ' በሎ።
1.196402
Sanali Adamu.
ንኣዳም ኣይኮነን።
1.196354
Sindilinso woyenera kutchedwa mwana wanu.
ደጊም ወድኻ ኽብሃል ኣይበቅዕን እየ።
1.196305
October 2015 _ Mafunso Atatu Omwe Anthu Amafuna Atafunsa Mulungu
, ጥቅምቲ 2015 _ ሰባት ንኣምላኽ ኪሓትትዎ ዚደልዩ 3 ሕቶታት
1.196275
16Kodi tsopano ine ndasanduka mdani wanu chifukwa ndakuwuzani choonadi?
16እሞኸ ሓቂ ስለ ዝነገርኩኹምዶ ጸላኢ ኾይነኩም እየ?
1.196164
"Kodi Umandikonda Ine Kuposa Izi?" - Yohane 21:15 _ Yophunzira
"ካብዚኣቶም ኣብሊጽካዶ ተፍቅረኒ ኢኻ፧" - ዮሃንስ 21:15 _ መጽናዕቲ
1.19616
Kodi Malemba amapereka malangizo otani kwa anthu olemera komanso osauka?
ቅዱሳት ጽሑፋት ንሃብታማት ኰነ ንድኻታት ዚህቦ ማዕዳ እንታይ እዩ፧
1.196129
6 2017 | Kodi Zinthu Padzikoli Zafika Poipa Kwambiri?
6 2017 | ዓለም ካብ ቍጽጽር ወጻኢ ድያ እትኸውን ዘላ፧
1.196091
PHUNZIRO 5 Mabwenzi a Mulungu Adzakhala M'paradaiso
ትምህርቲ 5 ኣዕሩኽ ኣምላኽ ኣብ ገነት ክነብሩ እዮም
1.196084
7 Akulu ena amavutika kukumbukira mayina.
7 ገሊኦም ሽማግለታት፡ ስም ምዝካር የጸግሞም እዩ።
1.195817
Mulungu ndiye pothawirapo ife."
ኣምላኽ መዕቈቢና እዩ።
1.195744
Kodi umadziŵa kuti nyenyezi zonse zili ndi mayina awo?
ከዋኽብቲ ብምሉኦም ስም ከም ዘለዎም ትፈልጥዶ፧
1.195699
Taonani ena mwa madalitso amene anthu amenewa adzasangalale nawo mu Ufumu wa Mulungu.
ገለ ኻብቲ ኣብ ትሕቲ መንግስቲ ኣምላኽ ኪፍጸም ዚጽበይዎ በረኸታት ንርአ።
1.195634
Mwachitsanzo, magazini ya September 2006 inali ndi mutu wakuti "Kodi Mlengi Alipo?"
ንኣብነት፡ ናይ መስከረም 2006 ሕታም፡ "ፈጣሪ ኣሎ ድዩ፧" ዚብል ኣርእስቲ ነበራ።
1.195632
Koma Mulungu anayang'ana mokoma mtima pa masautso anga ndi ntchito ya manja anga, ndipo adadzudzula inu dzulo. "
ኣምላኽ ግና መከራይን ጻዕሪ ኢደይን ረኣየ፣ ስለዚ ድማ እዩ ትማሊ ለይቲ ዝገንሓካ።
1.195617
Iye adzabweretsanso Aisraeli ambiri kwa Ambuye Mulungu wawo.
ንብዙሓት ህዝቢ እስራኤል ድማ ናብ ኣምላኾም ክመልሶም እዩ።
1.195605
maso awo ndi omatirira ndipo sangathe kuona,
ኣዒንቲ ኣለዎም፡ ግናኸ ኣይርእዩን፣
1.19559
Ndiponso ndikukulangizani; ndipo ndikudziwa zochokera kwa Allah zomwe inu simukuzidziwa."
ግን ከኣ ይኣኽለኒ ዘይትብሎ ፍልጠት ዜስተምህረካ።
1.19547
Iye atawira: 'Miti yonsene idakhonda kutcekwa na Baba wanga wakudzulu, iye anadzaidula.
ንሱ ኸኣ፡ "ሰማያዊ ኣቦይ ዘይተኸሎ ዘበለ ተኽሊ ኺምንቈስ እዩ።
1.195455
"Koma ukakonza phwando, uziitana anthu osauka, otsimphina, olumala, ndi akhungu.
ምሳሕ እንተ ገበርካስ፡ ድኻታትን ቈራያትን ሓንካሳትን ዕዉራትን ደኣ ጸውዕ።
1.1954
Muzipemphera musanayambe kuwerenga.
ቅድሚ ምንባብካ ጸሊ።
1.195339
Patulani iwo mchoonadi; mau anu ndi choonadi.
በቲ ሓቂ ቐድሶም፥ ቃልካ ሓቂ እዩ።
1.19525
22 Malamulo ake onse ali pamaso panga;
22 ኵሉ ፍርድታቱ ኣብ ቅድመይ እዩ፣
1.19523
11 "Mapeto a nthawi ino" anayamba mu 1914.
11 "መደምደምታ ስርዓት ዓለም" ብ1914 ጀመረ።
1.195101
Satana ndi mdani wa Mulungu, ndipo ndi mdani wathunso.
ሰይጣን ጸላኢ ኣምላኽ እዩ: ንዓናውን ጸላኢና እዩ።
1.195068
wopanda kupereka ndalama kapena mphotho,
ጻማ ዘይርከቦ ኣይ ሃብቲ ኣይክብረት:-
1.195045
Ndipo mchira wace uguza limodzi la magawo atatu a nyenyezi za m'mwamba, nuziponya padziko.
እቲ ጭራኡ ድማ ሲሶ ኸዋኽብቲ ሰማይ ሰሐበ፡ ናብ ምድሪውን ደርበዮም።
1.195007
Amafuna kuti mukhale ndi 'moyo weniweni.'
ነታ "ናይ ሓቂ ህይወት" ክትረኽባ ይደልየካ እዩ።
1.194985
Kodi bwanji sathokoza (Allah)?
ከመይጌርና (ብምንታይ) ከነመስግኖይግበኣና?
1.194794
Kwa ife, alipo Mulungu m'bodzi basi (5, 6)
ንዓና ሓደ ኣምላኽ ኣሎና (5, 6)
1.194735
Ndithu ine ndaitanira anthu anga (ku chikhulupiliro) usiku ndi usana (popanda kufooka)."
ዕለትየ ፡ ጸራኅኩ ፡ ኀቤከ ፡ ወሌሊትየኒ ፡ ቅድሜከ ።
1.194632
5 Tinazindikiranso kuti mbali yoyamba ya chisautso chachikulu sinayambe mu 1914.
5 ቀዳማይ ክፋል እቲ ብርቱዕ ጸበባ ብ1914 ከም ዘይጀመረ እውን ተገንዚብና ኢና።
1.194623
Pali pano, mumzinda wa New York muli mipingo 6 ya citundu ca Cirasha.
ሎሚ፡ ኣብ ከተማ ኒው ዮርክ ሽዱሽተ ጉባኤታት ሩስያኛ ኣለዋ።
1.194472
Chifukwa Inu nokha muli woyera: chifukwa mitundu yonse idzadza nidzalambira pamaso panu, popeza ziweruziro zanu zawonetsedwa.
እቲ ቕኑዕ ፍርድኻ ተግሂዱ እዩ እሞ ኲሎም ኣሕዛብ ክመጹ ኣብ ቅድሜኻዉን ክሰግዱ እዮም።
1.194377
Ndiyeno Yesu adzasangalala n'kuika kapoloyo pa udindo wake wachiwiri woyang'anira zinthu zake zonse.
ሽዑ የሱስ ተሓጒሱ ኣብ ኵሉ ንብረቱ ኺሸሞ እዩ፣ እዚ እቲ ኻልኣይ ሽመት እዩ።
1.194246
February 2014 _ Nkhondo Yomwe Inasintha Dziko Lonse
ለካቲት 2014 _ ንዓለም ዝቐየራ ውግእ
1.194246
Koma mlendo sizidzam'tsata, koma zidzam'thaŵa; chifukwa sizidziŵa mawu a alendo."
ድምጺ ኻልእ ዘይፈልጣ ስለ ዝዀና፡ ንኻልእ፡ ካብኡ ይገልባ እምበር፡ ኣይስዕባኦን እየን።
1.194172
14 Umboni woti limathandizidwa ndi angelo.
14 ሓገዝ መላእኽቲ።
1.194069
Gal 4:8 Komatu pajapo posadziwa Mulungu inu, mudachitira ukapolo iyo yosakhala milungu m'chibadwidwe chawo;
ቕድም ንኣምላኽ ከይፈለጥኩምዎ ኸሎኹም፥ ነቶም ብባህሪኦም ኣማልኽቲ ዘይኮኑ ብባርነት ትግዝኡ ነበርኩም።
1.193953
7 Werengani na mtima wakutsudzuka.
7 ብኽፉት ኣእምሮ ኣንብብ።
1.193828
12 Maganizo ndi mtima wake.
12 ኣብ መንፈሱን ኣብ ኣረኣእያኡን።
1.193813
Pafupifupi 500 mwa iwo ndi alongo osakwatiwa.
ካብዚኣቶም እተን 500 ንጽል ኣሓት እየን።
1.193799
Mngelo mbodzi adalonga kuna iwo mbati, "Lekani chita mantha Ine ndadza na mphangwa zadidi kuna imwe.
10 እቲ መልኣኽ ግና፡ "ንዅሉ ህዝቢ ዚኸውን ዓብዪ ሓጐስ አበስረኩም ኣለኹ እሞ፡ ኣይትፍርሁ።
1.193799
Ndipo padzaweruzidwa pakati pawo mwachoonadi, ndipo kudzanenedwa (ndi zolengedwa zonse): "Kuyamikidwa nkwa Allah, Mbuye wa zolengedwa!"
" ብዛዕባ ጎይትኡ ክዛረብ ከሎ ከኣ፣ "ደጊምሲ ጐይታይ፡ ንሱ እቲ ጻድቕ ፈራዲ" ክብሪ ንኣምላኽ ይኹን።
1.193796
Ndipo mutikhululukire ife machimo athu,
ንበደልና ይቕረታን ምሕረትን ግበረልና።
1.193642
Khalani na ndzidzi wakucedza pabodzi na anango, pontho citani masendzekero.
" ምስቶም ዚሕጎሱ ተሓጐሱ ምስቶም ዚበኽዩ ብኸዩ።
1.193603
ndidzati, "Mtendere ukhale mʼkati mwako."
"ሰላም ኣብ ውሽጥኺ ይኹን" ክብል እየ።
1.193508
October 2013 _ Zinthu Zitatu Zimene Sitingagule ndi Ndalama
ጥቅምቲ 2013 | ገንዘብ ኪዕድጎ ዘይክእል ሰለስተ ነገራት
1.193478
Izi zinachititsa kuti anthu ambiri akhale okhulupirira.
vብስብከቱ ድማ ብዙሓት አመኑ።
1.19337
Ndipo oipa adzachita zoipa, ndipo palibe woipa adzazindikira, koma ozindikira adzazindikira. "
+ እኩያት ከኣ እከይ ኪገብሩ እዮም፣ ካብቶም እኩያትሲ ሓደ እኳ ኣይኪርዳእን እዩ፣ እቶም ልቦና ዘለዎም ግና ኪርድኡ እዮም።
1.193255
Ayi ndithu, Iye ali kudzanja lamanja la Mulungu.
ኣብ የማን ኣምላኽ እዩ ተቐሚጡ ዘሎ ።
1.193193
Komabe palibe imodzi ya izo idzagwa pansi Atate wanu osadziwa ."
ሓንቲ እኳ ኻብኣተን ብዘይ ፍቓድ ሰማያዊ ኣቦኹም ኣብ ምድሪ ኣይትወድቕን እያ።
1.193188
Kuti tsopano mwakhala kudzanja lamanja la Mulungu Mulungu.
ኣብ የማን ኣምላኽ እዩ ተቐሚጡ ዘሎ ።
1.192934
6 2017 | Kodi Zinthu Padzikoli Zafika Poipa Kwambiri?
6 2017 _ ዓለም ካብ ቍጽጽር ወጻኢ ድያ እትኸውን ዘላ፧
1.192932
amene anapita kumwamba ndipo ali kudzanja lamanja la Mulungu komwe angelo ndi maulamuliro ndi amphamvu amamvera Iye.
22 - ንሱ ናብ ሰማይ ዐሪጉ ኣብ የማን ኣምላኽ ኣሎ፡ ንእኡ መላእኽትን ስልጣናትን ሓይልታትን ይግዝእዎ ኣለዉ።
1.192658
Adati, "Yesu, ndikumbukireni mukadzafika mu ufumu wanu."
ንኢየሱስ ከኣ ኦ ኢየሱስ ጐይታይ ብመንግስትኻ ኽትመጽኣ ከሎኻ ዘክረኒ በሎ።
1.192552
"Bulukani muna iye mbumba yanga" (4)
'ኣቱም ህዝበይ፡ ካብኣ ውጹ' (4)
1.192527
Tumikirani ndi mtima wonse, ngati kuti mukutumikira Ambuye, osati anthu.
7ንሰብ ዘይኮነስ ከም ንጐይታ እተገልግሉ ካብ ልቢ ኣገልግሉ።
1.192515
16Kodi tsopano ine ndasanduka mdani wanu chifukwa ndakuwuzani choonadi?
16 እሞ ደኣ፡ ሓቂ ስለ ዝነገርኩኹምዶ ጸላኢኹም ኰይነ እየ፧
1.192486
[39] 2 Musanthula m'malembo, popeza muyesa kuti momwemo muli nao moyo wosatha; ndipo akundicitira Ine umboni ndi iwo omwewo;[40] ndipo 3 simufuna kudza kwa Ine, kuti mukhale nao moyo.
39 - ናይ ዘለኣለም ህይወት በተን ጽሑፋት እትረኽቡ እናመሰለኩምሲ ትምርምርወን ኣሎኹም፡ ንሳተን ከኣ ብዛዕባይ እየን ዚምስክራ።
1.192266
Imbalimbisa ubale bwathu bwacikristau.
ንክርስትያናዊ ሕውነትና የደልድሎ።
1.192252
Ine ndili nacho chiyembekezo chomwecho chimene iwo ali nacho mwa Mulungu, kuti kudzakhala kuuka kwa akufa kwa olungama ndiponso kwa ochimwa.
15ከምቲ ንሳቶም ተስፋ ዝገብርዎ ኣነውን ጻድቃንን ኃጥኣንን ካብ ሞት ከም ዝትሥኡ ኣብ እግዚኣብሔር ተስፋ ኣለኒ።
1.192248
10Iye sadzabweranso ku nyumba kwake
10 ናብ ቤቱ መሊሱ ኣይምለስን፣
1.192227
Ana anu amaona kwambiri zimene mumachita.
ደቅኻ ነቲ እትገብሮ ይዕዘብዎ እዮም፣ እዚ ድማ ብርግጽ ጽቡቕ ጽልዋ ኺገብረሎም እዩ።
1.192059
Koma Yesu anati kwa iye, Undicha Ine wabwino bwanji? palibe wabwino, koma mmodzi, ndiye Mulungu.
የሱስ ድማ፡ "ስለምንታይ ሕያዋይ [ወይ፡ "ሰናይ"] እትብለኒ፧ ብዘይካ ሓደ ኣምላኽ፡ ሕያዋይ የልቦን" ኢሉ መለሰሉ።
1.192052
Iye aapfundzisambo toera kuphembera kuti dzina ya Mulungu iceneswe, Umambo wace udze, pontho toera cifuniro ca Mulungu cicitwe pa dziko yapantsi.
ብተወሳኺ ድማ፡ ስም ኣምላኽ ኪቕደስን መንግስቱ ኽትመጽእን ፍቓዱ ኣብ ምድሪ ኪኸውንን ኪጽልዩ መሃሮም።
1.191968
(pakuti cilamulo sicinacitira kanthu kakhale kopanda cirema), ndipo kulinso kulowa naco ciyembekezo coposa, cimene tiyandikira naco kwa Mulungu.
ሕጊ ንሓደ እኳ ኣብ ፍጻሜ ኣየብጽሖን፡ግናኸ ናብ ኣምላኽ እንቐርበላ፡ እትሐይሽ ተስፋ ኣተወት።
1.19175
Ndipo anati kwa iwo, Ndinaona Satana alinkugwa ngati mphezi wocokera kumwamba.
ኢየሱስ እውን "ሰይጣን ከም መብረቕ ካብ ሰማይ ኪወድቕ ከሎ ረአኽዎ" ኢልዎም።
1.191653
Iye anauza atumwi ake okhulupirika kuti: "Mupitiriza kukhala mabwenzi anga mukamachita zimene ndikukulamulani."
የሱስ ንሃዋርያቱ "ንስኻትኩም እዚ ዝአዘዝኩኹም ዘበለ ዅሉ እንተ ገበርኩም: ኣዕሩኸይ ኢኹም" በሎም።
1.191645
"Ndiponso sanganjate aliyense monga kunjata kwa iye (Allah).
አምላኽ ዘየፍቅሮ ሰብ የለን።
1.191578
Ndipo undiitane tsiku la cisautso: Ndidzakulanditsa, ndipo iwe udzandilemekeza.
"ብመዓልቲ ጸበባ ድማ ጸውዓኒ ፡ ኣነ ኸናግፈካ እየ ፡ ንስኻ'ውን ከተኽብረኒ ኢኻ ።
1.191494
Khalani tcheru; khazikikani mʼchikhulupiriro chanu; limbani mtima; khalani amphamvu.
ንቕሑ፡ ኣብ እምነት ጽንዑ፡ ሰብኡት ኩኑ በርትዑ።
1.191476
Kodi makolo angatsatire bwanji lemba la Yakobo 1:19?
ወለዲ ንያእቆብ 1:19 ኺትግብርዋ ዚኽእሉ ብኸመይ እዮም፧
1.191452
Kodi salinso Mulungu wa anthu a mitundu ina?
ናይ ኣሕዛብውን ኣምላኽዶ ኣይኮነን?
1.191427
Anafuna kuti iwo akhale ofunitsitsa kutumikira ena.
ንኻልኦት ኬገልግሉ ፍቓደኛታት ኪዀኑ እዩ ዚደልዮም ነይሩ።
1.191344
Koma cimfine ca ku Spain cinali ciyambi cabe.
ናይ ስጳኛ ኢንፍሉወንዛ ግና መጀመርታ ጥራይ እዩ ነይሩ።
1.191252
October 2015 _ Mafunso Atatu Omwe Anthu Amafuna Atafunsa Mulungu
ጥቅምቲ 2015 ሰባት ንኣምላኽ ኪሓትትዎ ዚደልዩ 3 ሕቶታት
1.191247
Zimene mumachita tsiku lililonse zingachititse kuti musangalatse Mulungu kapena ayi.
ኣብ መዓልታዊ ኣካይዳኻ፡ ንኣምላኽ ከተሐጕሶ ወይ ከተጕህዮ ትኽእል ኢኻ።
1.191195
ndi kukhazikitsa mzinda pochita zoyipa!
ድሕርዚ፡ ከተማ ጽድቂ፡ እምንቲ ኸተማ ኽትብሃሊ ኢኺ።
1.19105
Sitinamvere mawu anu, malamulo ndi malangizo anu amene munapereka kwa mtumiki wanu Mose.
ንሕና ኣዚና ንኣኻ ዐጊብና እቲ ንባርያኻ ሙሴ ዛአዘዝካዮ ትእዛዛትን ሕጋጋትን ፍርድታትን ድማ ኣይሐሎናዮን።
1.191028
5 Tayerekezerani kuti inuyo munali Asa.
5 ኣብ ቦታ ኣሳ ኸም ዘለኻ ጌርካ እሞ ሕሰብ።
1.191023
Kumeneko maonekedwe ake anasinthika pamaso pawo.
ኣብ ቅድሚኦም ትርኢቱ ተለወጠ።
1.19094
Tingapewe bwanji kukhala akapolo kwa anthu amalonda a m'dzikoli masiku ano?
ባሮት እቲ ኣብዚ ግዜ እዚ ዘሎ ናይ ንግዲ ዓለም ምእንቲ ኸይንኸውን እንታይ ኢና ኽንገብር እንኽእል፧
1.190919
Kunena zoona, nthawi ikubwera imene aliyense amene adzakuphani adzaganiza kuti akutumikira Mulungu.
አረ ዚቐትለኩም ዘበለስ ንኣምላኽ ኣገልግሎት የቕርበሉ ኸም ዘሎ ዚመስሎ ሰዓት ክትመጽእ እያ።
1.190905
Tiuzeni, Kodi Zinthu Izi Zidzachitika Liti?
"እስከ ንገረና፡ እዚ መዓስ ኪኸውን እዩ፧"
1.190873
8 Msonkhano wa Onse.
8 ህዝባዊ ኣኼባ።
1.190861
Pikhali Yezu na pyaka 12 pyakubalwa, acitambo mibvundzo.
የሱስ ገና ወዲ 12 ዓመት ከሎ፡ ከቢድ ሕቶታት ሓቲቱ እዩ።
1.190753
20 Ali kuti wanzeru?
20ጥበበኛ ደኣ ኣበይ ኣሎ?
1.190651
Umwi yulu wacimvizye Ciwa,
ንሰማያት ከኣ ብምስትውዓል ኣቘሞ።