score
float32 1.04
1.25
⌀ | Chichewa
stringlengths 10
497
| Tigrinya
stringlengths 10
498
⌀ |
|---|---|---|
1.218037
|
Ndipo itanani athandizi anu (kuti akuthandizeni) osakhala Allah; ngati inu mukunena zoona (kuti Qur'an njopekedwa).
|
ንኣምላኽ ከኣ፡ "ብሓቂ እንተ ኣሊኻ፡ በጃኻ ኽረኽበካ ሓግዘኒ" ኢሉ እናነብዐ ለመኖ።
|
1.217998
|
Tikudziwa kuti aliyense amene ndi mwana wa Mulungu sachimwirachimwirabe.
|
እቲ ካብ ኣምላኽ ዝተወልደ ኃጢኣት ከም ዘይገብር ንፈልጥ ኢና።
|
1.217864
|
Anango anakwanisa kulonga: 'Ife tisafunambo kuenda pabodzi na imwe, thangwi tabva kuti Mulungu ali na imwe.' - Zakariya 8:23.
|
ገሊኦም እሞ ኸኣ፡ "ኣምላኽ ምሳኻትኩም ከም ዘሎ ሰሚዕና ኢና እሞ፡ ምሳኻትኩም ክንከይድ ንደሊ ኢና" ኺብሉ እዮም።
|
1.217763
|
32 Ndipo adayankhula naye mawu a Ambuye, pamodzi ndi onse a mnyumba mwake.
|
32ንእኡን ንዂሎም እቶም ምስኡ ኣብ ገዝኡ ዝነበሩን ድማ ቃል እግዚኣብሔር ነገርዎም።
|
1.217633
|
4 Sathani alibe kulenga cinthu na cibodzico.
|
4 ሰይጣን ዋላ ሓንቲ ኣይፈጠረን።
|
1.217605
|
7 Ngakhale mtengo umakhala ndi chiyembekezo.
|
7 ኦም እኳ ተስፋ ኣለዎ።
|
1.217504
|
Ndipo iye anamanga mudzi, namutcha dzina lake ndi dzina la mwana wake, Enoch.
|
ንሱ ኸኣ ከተማ ሰርሔ፡ ስም እታ ኸተማ ድማ ብስም ወዱ ሄኖክ ኣውጽኣላ።
|
1.217444
|
4Anthu a mu mzindamo anagawikana; ena anali mbali ya Ayuda, ena mbali ya atumwi.
|
4 ህዝቢ እታ ኸተማ ግና ተመቕሉ፣ ገሊኣቶም ምስ ኣይሁድ፡ ገሊኣቶም ድማ ምስ ሃዋርያት ኰኑ።
|
1.217182
|
"Atate wanu wakumwamba amazidyetsa.
|
'ሰማያዊ ኣቦኹም እዩ ዚምግበን።
|
1.217106
|
Mwachitsanzo, Ufumu wa Mulungu usanakhazikitsidwe kumwamba, panali Akhristu ena odzozedwa amene anali kutumikira Mulungu mokhulupirika.
|
ንኣብነት፡ መንግስቲ ኣምላኽ ኣብ ሰማይ ቅድሚ ምምስራታ፡ ሓንቲ ጕጅለ እሙናት ቅቡኣት ክርስትያናት ንኣምላኽ ተገልግሎ ነበረት።
|
1.217044
|
Patapita zaka 12, tinakumananso ku New York.
|
ድሕሪ 12 ዓመት፡ ኣብ ኒው ዮርክ ዳግም ተራኸብና።
|
1.216886
|
Mulungu wakhala akuuza anthu uthenga wofunika pogwiritsa ntchito njira zosiyanasiyana.
|
ኣምላኽ ንሰባት ብእተፈላለየ መገዲ ገይሩ ኣገዳሲ መልእኽቲ ነጊርዎም እዩ።
|
1.216748
|
Zonse zimene chaonetsedwa ndi kuwala.
|
13ኲሉ ነገር እንተ ደኣ ናብ ብርሃን ቀሪቡ ግና ይርአ፤ እቲ ንዂሉ ከም ዝርአ ዝገብር ከዓ ብርሃን እዩ።
|
1.216715
|
Ngati ife timakhulupirira zimene Mulungu amanena, sitidzaopa akufa.
|
ነቲ ኣምላኽ ዝበሎ ንኣምነሉ እንተደኣ ዄንና: ምዉታት ኣይኬፍርሁናን እዮም።
|
1.2167
|
Koma atadza Iyeyo, Mzimu wa coonadi, adzatsogolera inu m'coonadi conse; pakuti sadzalankhula za iye mwini; koma zinthu ziri zonse adzazimva, adzazilankhula; ndipo zinthu zirinkudza adzakulalikirani.
|
እቲ መንፈስ ሓቂ ምስ መጸ ግና ናብ ኩሉ ሓቂ ዘበለ ኺመርሓኩም፤ ንሱ ነቲ ዝሰምዖ ዘበለ እዩ ዚዛረብ እምበር ካብ ርእሱ ኣይዛረብን እዩ።
|
1.216678
|
Mutsireledzi wanga ndi Ene,
|
ረዳእየይ ግን .
|
1.216526
|
Baibulo limati: "Pamene ana a Isiraeli anakaona, anati wina ndi mnzake, N'chiyani ichi?"
|
ደቂ እስራኤል ድማ እዚ ምስ ረኣዩ፡ እንታይ ምዃኑ ኣይፈለጡን እሞ፥ እዚ እንታይ እዩ፧ ኢሎም ንሓድሕዶም ተሓታትቱ።
|
1.216318
|
13 Tizilankhula nawo mofatsa.
|
13 ብልእመት ተዛረብ።
|
1.216267
|
Ndiponso sindinkadziwa kuti Mulungu analengeranji dziko lapansili komanso anthu.
|
ብዛዕባ እቲ ኣምላኽ ንምድሪ ወይ ንደቂ ሰብ ዘለዎ ዕላማ ዋላ ሓንቲ ፍልጠት ኣይነበረንን።
|
1.216208
|
Kunena zoona, nthawi ikubwera imene aliyense amene adzakuphani adzaganiza kuti akutumikira Mulungu.
|
ካብ ቤት ጸሎቶም ኬውፅኡኹም እዮም፥ አረ እቲ ዚቐትለኩም ዘበለስ ንኣምላኽ ኣገልግሎት ዜቕርበሉ ኸም ዘሎ ዚመስሎ ጊዜ ኽትመጽእ እያ።
|
1.216098
|
Munthu woyambirira Adamu anakhala ndi moyo kwa zaka zambiri.
|
እቲ ቐዳማይ ሰብ ዝዀነ ኣዳም ንዘመናት ብህይወት ነይሩ እዩ።
|
1.215807
|
Iwo amalengeza uthenga wabwino ndiponso amathandiza anthu kulengeza uthengawo.
|
ከመይሲ፡ ባዕላቶም ብስራት ይነግሩ፡ ንኻልኦት ሰባት እውን ብስራት ንኺዝርግሑ ይድግፍዎም እዮም።
|
1.215419
|
Baibulo limatiuza kuti: "[Mulungu] anakhazika dziko lapansi pa maziko ake, silidzagwedezeka ku nthawi yonse."
|
መጽሓፍ ቅዱስ፡ "[ኣምላኽ] ንዘለኣለም ከይትናወጽሲ፡ ንምድሪ ኣብ መሰረታ ኣጽንዓ" ይብል።
|
1.215245
|
Koma atadza Iyeyo, Mzimu wa choonadi, adzatsogolera inu m'choonadi chonse; pakuti sadzalankhula za Iye mwini; koma zinthu zilizonse adzazimva, adzazilankhula; ndipo zinthu zilinkudza adzakulalikirani.
|
እቲ መንፈስ ሓቂ ምስ መጸ ግና ናብ ኩሉ ሓቂ ዘበለ ኺመርሓኩም፤ ንሱ ነቲ ዝሰምዖ ዘበለ እዩ ዚዛረብ እምበር ካብ ርእሱ ኣይዛረብን እዩ።
|
1.215234
|
18 Tonse tikhoza kutsatira mfundo ya m'mawu a Paulowa.
|
18 ኵላትና ነቲ ኣብ ቃላት ጳውሎስ ዚርከብ መሰረታዊ ስርዓት ክንትግብሮ ንኽእል ኢና።
|
1.215117
|
"Ndipo mapiri adzakhala ngati ubweya womwazidwa (wongouluka uku ndi uku mumlengalenga).
|
ኣኽራን ከም ደዓውል፡ ኰረቢት ከም ዕያውቲ ተሰራሰሩ።
|
1.215096
|
"Ndikupanga Zinthu Zonse Kukhala Zatsopano" 147.
|
"ንዅሉ እሕድሶ ኣለኹ" 147.
|
1.214546
|
Kodi ndani ali wabwino poweruza kuposa Allah kwa anthu otsimikiza (kuti Allah alipo)?
|
ዝገደደ ኸኣ ካብ ኣምላኽ እንቕበሎ ፍርዲ ዓቢ ይኸውን።
|
1.214504
|
2 Yesu sanachite mantha.
|
2 የሱስ ግን ኣይፈርሀን።
|
1.214445
|
Kodi mukudziwa njira imene Mulungu amagwiritsa ntchito akafuna kulankhula nafe?
|
ኣምላኽ ብኸመይ ከም ዚዛረበና ትፈልጥዶ፧
|
1.214435
|
Kwa zaka 17 ndinkapemphera kuti ndipeze mayankho a mafunso anga.
|
መልሲ ሕቶታተይ ንምርካብ ንልዕሊ 17 ዓመት ጸልየ እየ።
|
1.214246
|
35 Ndipo iye amene adawona, wachita umboni, ndi umboni wake uli wowona; ndipo iyeyu adziwa kuti anena zowona, kuti inunso mukakhulupirire.
|
35 እቲ ነዚ ዝረኣየ ድማ መስከረ፣ ምስክሩ ኸኣ ሓቂ እዩ፣ ንስኻትኩም እውን ምእንቲ ኽትኣምኑ ኸኣ፡ ንሱ ሓቂ ኸም ዝነገረ ይፈልጥ እዩ።
|
1.214245
|
Ndipo njira yanu inadutsa pamadzi ambiri.
|
መገድኻ ኣብ ብዙሕ ማያት እዩ ነይሩ፣
|
1.214143
|
Atumwi ankakhulupirira ndi mtima wonse kuti akufa adzauka.
|
ሃዋርያት ብዛዕባ ትንሳኤ ምዉታት ኣጸቢቖም ይኣምኑ ነበሩ።
|
1.213928
|
Titeteze Mitima Yathu 37.
|
ንልብና ንሓልዎ 37.
|
1.213871
|
Iye anaphunzira zinthu zambiri kwa Atate wake ndipo ankaziyamikira kwambiri.
|
ካብ ኣቦኡ ብዙሕ እዩ ተቐቢሉ፣ ነቲ እተቐበሎ ድማ ብሓቂ ኣኽቢሩ ይርእዮ ነበረ።
|
1.213846
|
Mulungu sangamve mapemphero athu ngati tilibe chikhulupiriro.
|
ብዘይ እምነት ንኣምላኽ ብጸሎት ክንቀርቦ ኣይንኽእልን ኢና።
|
1.21338
|
Ngati akanasankha kumvera Mulungu, akanakhala ndi moyo wosatha m'Paradaiso.
|
ኣዳም ንኣምላኽ ኪእዘዝ እንተ ዚመርጽ፡ ኣብ ገነት ንዘለኣለም ኪነብር ምኸኣለ ነይሩ።
|
1.213357
|
Inenso ndine Mwisiraeli.
|
ኣነውን እስራኤላዊ እየ።
|
1.213269
|
"Tamverani Maloto Amene Ine Ndinalota"
|
"ዝሐለምክዎ ሕልሚ እማ ስምዑ"
|
1.213124
|
uthenga umene amalalikira komanso chifukwa chake amalalikira?
|
ዚሰብክዎ መልእኽትን ስለምንታይ ከም ዚሰብክዎን
|
1.213065
|
Wakuitana inu ali wokhulupirika, amenenso adzachichita.
|
እቲ ዚጽውዓኩም ዘሎ እሙን እዩ፡ ንሱውን ኪገብሮ እዩ።
|
1.212959
|
(Tidampititsa kumeneko) kuti timsonyeze zina mwa zisonyezo Zathu; ndithu Iye (Allah) Ngwakumva, Ngowona (chilichonse).
|
'እቲ ዘይርአ ባህርዩ፡ ብንጹር ይርአ'
|
1.212835
|
Amapereka moyo ku zinthu zonse.
|
ንሱ ንዅሉ ሰብ ሕይወትን ትንፋስን ኵሉ ነገርን ዚህብ እዩ።
|
1.212742
|
18Yosefe anati, "Tanthauzo lake ndi ili: nsengwa zitatuzo ndi masiku atatu.
|
18 ዮሴፍ ከኣ ከምዚ ኢሉ መለሰሉ፦ "ትርጉሙ እዚ እዩ፦ እቲ ሰለስተ መሶብ፡ ሰለስተ መዓልቲ እዩ።
|
1.212566
|
Mulungu anapatsa dzina munthu wamwamuna woyamba kukhala padziko lapansi.
|
ኣምላኽ ነቲ ኣብ ምድሪ ዝፈጠሮ ናይ መጀመርታ ሰብኣይ ስም ኣውጺኡሉ እዩ።
|
1.212431
|
15 Tizikhululuka ndi mtima wonse.
|
15 ብናጻ ይቕረ በል።
|
1.212374
|
15 Iwe udzakhala mboni yake kwa anthu onse pa zimene waziona ndi kuzimva.
|
15እዙይ ድማ በቲ ዝረአኻዮን ዝሰማዕኻዮን ኣብ ኲሉ ሰብ ምስክር ምእንቲ ኽትኮኖ እዩ።
|
1.212343
|
Act 14:4 Ndipo khamu la mumzinda lidagawikana; ena adali ndi Ayuda koma ena adali ndi atumwi.
|
4 ህዝቢ እታ ኸተማ ግና ተመቕሉ፣ ገሊኣቶም ምስ ኣይሁድ፡ ገሊኣቶም ድማ ምስ ሃዋርያት ኰኑ።
|
1.212316
|
Solomo anali munthu wolemera kwambiri.
|
� ሰሎሞን ሃብቶም፡
|
1.212299
|
Iye anati: "Kudwala kumeneku si kwa imfa chabe, koma n'kopatsa Mulungu ulemerero, kuti mwa kudwalako, Mwana wa Mulungu alemekezeke."
|
ብዛዕባ እዚ ኺገልጽ ከሎ ድማ፡ "እዚ ሕማም እዚ፡ ወዲ ኣምላኽ ብእኡ ምእንቲ ኪኸብር፡ ንኽብሪ ኣምላኽ እዩ እምበር፡ ንሞት ኣይኰነን" በለ።
|
1.212219
|
Joh 5:39 Musanthula m'malembo, popeza muyesa kuti momwemo muli nawo moyo wosatha; ndipo akundichitira Ine umboni ndi iwo omwewo;
|
39 - ናይ ዘለኣለም ህይወት በተን ጽሑፋት እትረኽቡ እናመሰለኩምሲ ትምርምርወን ኣሎኹም፡ ንሳተን ከኣ ብዛዕባይ እየን ዚምስክራ።
|
1.212108
|
ndipo ndinayitana mwana wanga kuti atuluke mu Igupto.
|
ንወደይ ካብ ግብጺ ጸዊዐዮ።
|
1.211936
|
Ndi bugu ifhio ya dzipsalme ine ya sumbedza nḓila ine Mudzimu a thusa na u khuthadza ngayo vhane vha mu funa?
|
ኣምላኽ ብምምካርን ብምግሳጽን ፍቕሩ ዘርኣየ ብኸመይ እዩ፧
|
1.211735
|
"Mwezi wopatulika kwa mwezi wopatulika; ndipo zinthu zopatulika paikidwa kubwezerana.
|
እታ ዝተቐደሰት እስላማዊት ወርሒ ተገይራ ኸኣ ትውሰድ።
|
1.211666
|
"Tiuzeni, Kodi Zinthu Zimenezi Zidzachitika Liti?"
|
"እስከ ንገረና፡ እዚ መዓስ ኪኸውን እዩ፧"
|
1.211586
|
January 2015: Kodi Moyo Unayamba Bwanji?
|
፡ ጥሪ 2015፦ ህይወት ብኸመይ ጀሚሩ፧
|
1.211511
|
"Ndipo mapiri adzakhala ngati ubweya womwazidwa (wongouluka uku ndi uku mumlengalenga).
|
ኣኽራን ከም ደዓውል፣ ኰረቢት ከም ዕያውቲ ተሰራሰሩ።
|
1.211403
|
Anthu okonda Mawu a Mulungu anazindikira mfundo imeneyi kalekale.
|
እቶም ቃል ኣምላኽ ዚፈትዉ ዘበሉ ነዚ ሓቂ እዚ ሓቂ እዚ ኻብ ዚርድእዎ ነዊሕ ገይሮም እዮም።
|
1.211309
|
"Kodi Undikonda Ine Koposa Awa?"
|
"ካብዚኣቶም ኣብሊጽካዶ ተፍቅረኒ ኢኻ፧"
|
1.211273
|
Pemphelo la Mtumiki wa Mulungu 43.
|
ጸሎት ኣገልጋሊ ኣምላኽ 43.
|
1.211204
|
Pemphero la Mtumiki wa Mulungu 43.
|
ጸሎት ኣገልጋሊ ኣምላኽ 43.
|
1.211148
|
kungakuthandizeni bwanji kuti musamaope anthu?
|
ካብ ፍርሂ ሰብ ዜዕቝበካ ብኸመይ እዩ፧
|
1.210828
|
8 Cedzani na anthu.
|
8 ንሰባት ምዝርራብ።
|
1.210745
|
3Ngodala munthu amene awerenga mawu oneneratu zamʼtsogolo ndi iwo amene amamva ndi kusunga zolembedwa mʼbukuli pakuti nthawi yayandikira.
|
3እቲ እዙይ ዝፍጸመሉ ዘመን ቀረባ ስለ ዝኾነ ድማ እቲ ነዝ ቓል ትንቢት እዙይ ዘንብብ ብፁዕ እዩ፤ እቶም ዝሰምዕዎን ነቲ ኣብኡ ተጽሒፉ ዘሎ ዝፍጽምዎንውን ብፁዓን እዮም።
|
1.21057
|
Inu munakantha mitundu ya anthu,
|
ነቲ ህዝቢ ኣዕቢኻዮ፣
|
1.210441
|
Akweze mawu ako ngati lipenga, ndi kulengeza kuti anthu anga zochita zawo zoipa, ndi banja la Yakobo machimo awo.
|
ንህዝበይ ዕልወቶም፡ንቤት ያእቆብ ድማ ሓጢኣቶም ንገሮም።
|
1.210388
|
Ndiponso Mose awauza kuti: 'Munthu aliyense asasiyeko mana akuti akadye tsiku lotsatila.'
|
ሙሴ ድማ፡ ሓደ እኳ ኻብኡ ገለ ኽሳዕ ንጽብሒቱ ኣየትርፍ፡ በሎም።
|
1.210303
|
Izi zinandithandiza kuti ndiziwamvera.
|
እዚ ድማ እዙዝ ኪኸውን ሓጊዙኒ እዩ።
|
1.210252
|
"Kodi Umandikonda Ine Kuposa Izi?"
|
"ካብዚኣቶም ኣብሊጽካዶ ተፍቅረኒ ኢኻ፧"
|
1.210208
|
Basi pa tsikuli okhulupirira adzaseka
|
ቀንም ምእመናን ይደሰታሉ።
|
1.209978
|
ndi chimwemwe kwa olungama mtima.
|
ነቶም ቅኑዕ ዝልቦም ከኣ ሓጐስ ኰይኑሎም።
|
1.209905
|
"Ndipo ndili ndi chiyembekezo kwa Mulungu, chomwe chiyembekezo chaninso awa akuyembekeza, kuti chidzakhala chiwukitsiro cha onse olungama ndi osalungama. "
|
15ከምቲ ንሳቶም ተስፋ ዝገብርዎ ኣነውን ጻድቃንን ኃጥኣንን ካብ ሞት ከም ዝትሥኡ ኣብ እግዚኣብሔር ተስፋ ኣለኒ።
|
1.209858
|
Iye anati: "Atate, ngati mukufuna, ndicotseleni kapu iyi.
|
ሽዑ፡ "ኣቦ፡ እንተ ፈቲኻስ፡ ነዛ ጽዋእ እዚኣ ኻባይ ኣልግሳ።
|
1.209805
|
kapolo wokhulupirira ndi wanzeru 111
|
እሙንን ኣስተውዓልን ባርያ 111
|
1.209519
|
9 Kodi sindine mfulu?+ Kodi sindine mtumwi?+ Kodi sindinaone Yesu Ambuye wathu?+ Kodi inu sindinu ntchito yanga mwa Ambuye?
|
9 ሓራ ደይኰንኩን፧ ሃዋርያ ደይኰንኩን፧ ንጐይታና የሱስ ክርስቶስከ ኣይረኣኽዎን ድየ፧+ ንስኻትኩምከ ብጐይታ ዕዮይ ደይኰንኩምን፧
|
1.209309
|
Na tenepo, Juwau acemera axamwali ace awiri, mbaatuma kuna Yezu na cibvunzo ici: " Iwe ndiwedi ule adabuluka kuna Mulungu, peno tinasaka unango? "
|
ስለዚ፡ ንኽልተ ደቀ መዛሙርቱ ጸዊዑ፡ "እቲ ዚመጽእሲ ንስኻ ዲኻ፡ ወይስ ካልእ ክንጽበ ኢና፧" ኢሉ ናብ የሱስ ለኣኾም።
|
1.209176
|
ndipo ndinapenya mphamvu zanu ndi ulemerero wanu.
|
ብርታዐኻን ክብርኻን ድማ ርእየ።
|
1.209151
|
Cifukwa cace, taonani, nditumiza kwa inu aneneri ndi anzeru ndi alembi.
|
"ስለዚ እንሆ፡ ነብያት ጠቢባንን ጸሓፍትን እልእከልኩም አሎኹ።
|
1.209143
|
Ili kuti mvula yakupatsa Kwanu,
|
በቲ ነዃል ከኣ ዝናብ ይኣቱ።
|
1.20912
|
Tsono Malamulo sangathe kusandutsa chilichonse kukhala changwiro, koma mʼmalo mwake mwalowa chiyembekezo chabwino, chimenechi timayandikira nacho kwa Mulungu.
|
ሕጊ ንሓደ እኳ ኣብ ፍጻሜ ኣየብጽሖን፡ግናኸ ናብ ኣምላኽ እንቐርበላ፡ እትሐይሽ ተስፋ ኣተወት።
|
1.209032
|
Ndipo amene wamfuna amamuika pa njira yolunjika (yomwe ndi njira ya Chisilamu).
|
ንሶም ድማ፡ ንዝደለይዎ ሰብ ይዕድሉ።
|
1.209025
|
Umenewutu ndi mwayi waukulu kwambiri kwa iwowo komanso ifeyo.
|
እዝስ ንዓታቶም ኰነ ንዓና ኣየ ኸመይ ዝበለ ፍሉይ መሰል ኰን እዩ!
|
1.208982
|
Timafunika Kukhala Odziletsa 122.
|
ርእስና ኽንገትእ ኣሎና 122.
|
1.20897
|
Tachita chosalungama pamaso panu, sitinakhonza kumvera malamulo anu mulungu amene munamupatsa kapolo wanu Mose."
|
ንሕና ኣዚና ንኣኻ ዐጊብና እቲ ንባርያኻ ሙሴ ዛአዘዝካዮ ትእዛዛትን ሕጋጋትን ፍርድታትን ድማ ኣይሐሎናዮን።
|
1.208725
|
Iye anati: "Akakuzunzani mumzinda wina, muthawire mumzinda wina."
|
ስለዚ ድማ፡ "ካብ ሓንቲ ኸተማ እንተ ሰጒጎምኹም፡ ናብ ካልእ ህደሙ" ኢሉ ተዛሪቡ እዩ።
|
1.208718
|
8 Dalirani Iye nthawi zonse, inu anthu;
|
8 ኣቱም ህዝቢ፡ ኵሉ ግዜ ብእኡ ተኣመኑ።
|
1.208564
|
Sitipatsidwa malipiro ena alionse tikamalalikira, kuphunzitsa mumpingo kapena tikamamanga nyumba zolambiriramo.
|
ንኽንሰብኽ፡ ኣብ ጉባኤ ንኽንምህር፡ ወይ ከኣ ቦታታት ኣምልኾ ንኽንሃንጽ ኣይንኽፈልን ኢና።
|
1.208341
|
Izi zikusonyeza kuti Abulahamu ankakhulupirira kuti akufa adzaukitsidwa.
|
' እወ፡ ኣብርሃም ብትንሳኤ ይኣምን ነይሩ እዩ።
|
1.20811
|
13 Anthu adziwa dzina la Mulungu kuyambira pamene analengedwa.
|
13 ሰባት ንስም ኣምላኽ ካብ እዋን ፍጥረት ኣትሒዞም ይፈልጥዎ ነይሮም እዮም።
|
1.207965
|
North America - Tsiku la Anthu Akufa
|
ሰሜን ኣመሪካ - መዓልቲ ምዉታት
|
1.207557
|
Pa nthawi imeneyi n'kuti inenso nditabwerera ku Hong Kong.
|
ኣብቲ ግዜ እቲ፡ ኣነ እውን ኣብ ሆንግ ኮንግ እየ ዝቕመጥ ነይረ።
|
1.20755
|
Tikhale Oyera M'makhalidwe Athu Onse
|
ብዅሉ ኣካይዳና ቕዱሳት ክንከውን ይግብኣና
|
1.207369
|
Mulungu amasangalala ndi anthu amene amafunadi kumutumikira ndi mtima wonse.
|
እቲ ነቶም ብልቢ ዝደልይዎ ኣብ ቀረባ ዝርከብ ኣምላኽ።
|
1.207367
|
Mwachitsanzo, m'chaputala 4 anafotokoza za Abulahamu.
|
ኣብ ምዕራፍ 4፡ ብዛዕባ ኣብርሃም ገሊጹ እዩ።
|
1.207044
|
Leka 'Kufunafuna Zinthu Zazikulu'
|
"ንርእስኻ ዓበይቲ ነገራት" ኣይትድለ
|
1.207024
|
Pitirizani Kufunafuna Ufumu Choyamba 22.
|
ቅድም መንግስቲ ኣምላኽ ድለዩ 22.
|
1.206964
|
Natenepa Yezu aphembera 'tayu basi thangwi ya awa [ale akhali cifupi na iye], mbwenye ndisakuphembanimbo thangwi ya ale anafuna kundikhulupira kubulukira ku mafala awo.'
|
ስለዚ ድማ፡ የሱስ፡ "ምእንቲ እቶም ብቓሎም ብኣይ ዚኣምኑ እውን እምበር፡ ምእንቲ እዚኣቶም [እቶም ኣብኡ ዝነበሩ] ጥራይ ኣይኰንኩን ዝልምን ዘለኹ" ኢሉ ጸለየ።
|
1.206896
|
"Ndithudi, m'kulenga kwa kumwamba ndi dziko lapansi ndi kusinthana kwa usiku ndi usana, muli zisonyezo kwa eni nzeru,
|
"ሰማያትንና ምድርን ብምፍጣር ምሽትን ቀትርን ብምትክካእ ንበዓል አእምሮታት ብርግፅ ምልክታት አለው።
|
1.206832
|
8 Tizikonda adani athu.
|
8 ጸላኢኻ ኣፍቅር።
|
Subsets and Splits
No community queries yet
The top public SQL queries from the community will appear here once available.