score
float32 1.04
1.25
⌀ | Chichewa
stringlengths 10
497
| Tigrinya
stringlengths 10
498
⌀ |
|---|---|---|
1.249439
|
Mungatowezera cikhulupiro ca Nowa, munakwanisambo kupulumusa umaso wanu na wa ale anafuna imwe.
|
ኣስኣሰር እምነት ኖህ እንተ ስዒብካ፡ ንስኻ እውን ንርእስኻን ነቶም እትፈትዎምን ከተድሕን ትኽእል ኢኻ።
|
1.249424
|
46 Penepo, mbuya wace anadza kabwera ntsiku ikhakhonda iye kudikhira, pa n'dzidzi unakhonda iye kudziwa.
|
ጐይታ እቲ ባርያ እቲ፡ ንሱ ብዘይተጸበያ መዓልቲ ብዘይፈላጣ ጊዜውን ኪመጽእ እዩ።
|
1.247489
|
Ndinu kulima Mulungu; ndinu yomanga Mulungu.
|
ንስኻትኩም ሕርሻ ኣምላኽ፡ ህንጻ ኣምላኽ ኢኹም።
|
1.247311
|
64 Koma pali ena mwa inu amene sakukhulupirira."
|
64 ገለ ኻባኻትኩም ግና ዘይኣምኑ ኣለዉ" በሎም።
|
1.246644
|
Komatu palibe ngakhale imodzi imene idzagwa pansi Atate wanu osadziwa."
|
ሓንቲ እኳ ኻብኣተን ብዘይ ፍቓድ ሰማያዊ ኣቦኹም ኣብ ምድሪ ኣይትወድቕን እያ።
|
1.246618
|
9Iye sanasiyanitse pakati pa ife ndi iwo, pakuti anayeretsa mitima yawo mwachikhulupiriro.
|
9ልቦም ብእምነት ስለ ዘንጽሀ ኣብ መንጎናን ኣብ መንጎኣቶምን ሓንቲ እኳ ኣይፈላለየን።
|
1.246501
|
M'malomwake ananena kuti: "Kudwala kumeneku si kwa imfa chabe, koma n'kopatsa Mulungu ulemerero, kuti mwa kudwalako, Mwana wa Mulungu alemekezeke."
|
የግዳስ፡ "እዚ ሕማም እዚ፡ ወዲ ኣምላኽ ብእኡ ምእንቲ ኪኸብር፡ ንኽብሪ ኣምላኽ እዩ እምበር፡ ንሞት ኣይኰነን" በለ።
|
1.246326
|
Ngati nanunso mutatsanzira chikhulupiriro cha Nowa, zingathandize kuti inuyo ndi banja lanu mudzapulumuke.
|
ኣስኣሰር እምነት ኖህ እንተ ስዒብካ፡ ንስኻ እውን ንርእስኻን ነቶም እትፈትዎምን ከተድሕን ትኽእል ኢኻ።
|
1.24526
|
Musamaope munthu aliyense, pakuti chiweruzo ndi cha Mulungu.
|
ፍርዲ ናይ ኣምላኽ እዩ እሞ፡ ገጽ ሰብ ኣይትፍርሁ።
|
1.244964
|
Ngati nanunso mutatsanzira chikhulupiriro cha Nowa, zingathandize kuti inuyo komanso banja lanu mudzapulumuke.
|
ኣስኣሰር እምነት ኖህ እንተ ስዒብካ፡ ንስኻ እውን ንርእስኻን ነቶም እትፈትዎምን ከተድሕን ትኽእል ኢኻ።
|
1.244627
|
Ngakhale atakuchimwirani kasanu ndi kawiri patsiku ndipo abwereranso kwa inu maulendo asanu ndi awiri nati, 'Ndalapa,' muyenera kuwakhululukira.
|
ኣብ መዓልቲ ሸውዓተ ሳዕ እኳ እንተ በደለካ፡ 'ተጣዒሰ' እናበለ ኸኣ ሸውዓተ ሳዕ ናባኻ እንተ ተመሊሱ፡ ሕደገሉ።
|
1.243392
|
Tsopano ife tikudziwa kuti chiweruzo cha Mulungu, chotsutsa amene amachita zinthu zotere, nʼchokhazikika pa choonadi.
|
"ንሕናስ ኣብቶም ከምዚ ዝበለ ዚገብሩ እቲ ፍርዲ ኣምላኽ ሓቂ ምዃኑ ንፈልጥ ኢና።
|
1.242349
|
35 Ndipo iye adati kwa iwo, amuna inu a Israyeli, tamachenjerani mwa inunokha za anthu awa, chimene muti muwachitire.
|
35 በሎም ድማ፡ኣቱም ሰብ እስራኤል፡ ኣብዞም ሰባት እዚኣቶም ክትገብርዎ እትሐስብዎ ዘሎኸም ተጠንቀቑሉ።
|
1.242081
|
44 Koma iwo adaganiza kuti Iye adali m'chipilingu cha ulendo, nayenda ulendo wa tsiku limodzi; ndipo adayamba kumfunafuna Iye mwa abale awo ndi mwa anansi awo.
|
ምስ ሰብ መገዲ ዘሎ መሲልዎም፡ መገዲ ሓንቲ መዓልቲ ኸዱ፡ ኣብ ኣዝማዶምን ኣብ ዚፈልጥዎምን ከኣ ደለይዎ።
|
1.241795
|
15Anati kwa iwo, "Pitani mʼdziko lonse lapansi ndipo mukalalikire Uthenga Wabwino kwa zolengedwa zonse.
|
15 ከምዚ ድማ በሎም፦ "ናብ ኵላ ዓለም ኪዱ፡ ንዅሉ ፍጥረት ከኣ ብስራት ስበኹሉ።
|
1.241614
|
4 Ngakhale akuchimwire maulendo 7 pa tsiku, n'kubwera kwa iwe maulendo 7, kudzanena kuti, 'Ndalapa ine,' umukhululukire ndithu."+
|
ኣብ መዓልቲ ሸውዓተ ሳዕ እኳ እንተ በደለካ፡ 'ተጣዒሰ' እናበለ ኸኣ ሸውዓተ ሳዕ ናባኻ እንተ ተመሊሱ፡ ሕደገሉ።
|
1.241266
|
Koma anapulumutsa Loti wolungamayo, amene anavutika mtima kwambiri ndi anthu ophwanya malamulo, mwa kulowerera kwawo khalidwe lotayirira."
|
ነቲ ብኣበሳኦምን ብርኹስ ንብረቶምን ዚስቀ ዝነበረ ሎጥ ጻድቕ ግና ኣድሐኖ፡
|
1.240969
|
Umenewu ndi ubwino wa Allah; amaupereka kwa amene wamfuna.
|
ንዘደለዮ ልዕል ኣበሎ፣ ንዝደለዮ ኸኣ ኣዋረዶ።
|
1.240178
|
Ngakhale atakuchimwirani kasanu ndi kawiri pa tsiku, ndikubwereranso maulendo asanu ndi awiri nkunena kuti, 'Ndalapa,' muyenera kuwakhululukira. "
|
ኣብ መዓልቲ ሸውዓተ ሳዕ እኳ እንተ በደለካ፡ 'ተጣዒሰ' እናበለ ኸኣ ሸውዓተ ሳዕ ናባኻ እንተ ተመሊሱ፡ ሕደገሉ።
|
1.240148
|
Mpostolo Juwau adanemba kuti: 'Ule omwe an'khulupira Mwanayo ana moyo wakusaya kumala, omwe an'khulupira lini Mwanayo an'dzaugumana lini moyo, koma ukali bwa Mulungu bun'dzakhala pa iye.'
|
ሃዋርያ ዮሃንስ፡ "እቲ ብወዲ ዚኣምን፡ ናይ ዘለኣለም ህይወት ኣላቶ፣ እቲ ንወዲ ዘይእዘዞ ግና፡ ቍጥዓ ኣምላኽ ደኣ ኣብኡ ይነብር እምበር፡ ንህይወት ኣይኪርእያን እዩ" ኢሉ ጸሓፈ።
|
1.239902
|
Kenako ananena kuti: "Choncho pitani mukaphunzitse anthu a mitundu yonse."
|
ሽዑ ድማ፡ 'ኪዱ ኻብ ኵሎም ኣህዛብ ደቀ መዛሙርቲ ግበሩ።
|
1.239586
|
Allah ndiye Wamkulu kuposa iwo amunawo.
|
ኣምላኽ ካብ መዋቲ ሰብ ኣጸቢቑ ይዓቢ እዩ።
|
1.239152
|
Limati: "Yehova ali pafupi ndi onse oitanira pa iye.
|
"የሆዋ ንዅሎም እቶም ዚጽውዕዎ፡ ንዅሎም እቶም ብሓቂ ዚጽውዕዎ ቐረባኦም እዩ።
|
1.237798
|
Ngakhale anthu amene amapita kutchalitchi sadziwa bwinobwino Malemba.
|
መብዛሕትኦም እቶም ሃይማኖተኛታት ዚብሃሉ እውን እንተ ዀኑ፡ ብዛዕባ ቕዱሳት ጽሑፋት ሒደት ፍልጠት እዩ ዘለዎም።
|
1.237533
|
January 2013 _ Kodi Muyenera Kuopa Kutha kwa Dzikoli?
|
ጥሪ 2013 መወዳእታ ዓለም ኬፍርሃካ ይግባእዶ፧
|
1.237508
|
5 Farao anati kwa Yosefe, "Abambo ako ndi abale ako abwera kwa iwe.
|
5 ፈርኦን ድማ ንዮሴፍ፤ ኣቦኻን ኣሕዋትካን መጺኦምኻ።
|
1.237334
|
Pakuti anthu wochimwa amachitanso chomwecho.
|
ከምኡስ ኃጥኣንውን ይገብሩ እዮም።
|
1.237263
|
Khalani Wokhululuka 131.
|
ይቕረ በሃልቲ ንኹን 131.
|
1.237217
|
Anapita nawo kumpoto ndi kum'mawa.
|
ናብ ሰሜንን ናብ ምብራቕን ተወስዱ
|
1.235383
|
Popeza iwo asankha njira zawozawo,
|
መገድታት ርእሶም ሓርዮም፣
|
1.235067
|
maso ali nawo, koma sapenya;
|
ኣዒንቲ ኣለዎም፡ ግናኸ ኣይርእዩን፣
|
1.234795
|
Iye adzakhala wamkulu ndipo adzatchedwa Mwana wa Wammwambamwamba.
|
ንሱ ዓብዪ ኪኸውን፡ ወዲ እቲ ልዑል እውን ኪብሃል እዩ፣ .
|
1.234284
|
Mtumwi Paulo ananenanso kuti "olungama ndi osalungama omwe" adzaukitsidwa.
|
ሃዋርያ ጳውሎስ እውን፡ "ንጻድቃንን ንሓጥኣንን" ትንሳኤ ኸም ዚኸውን ገሊጹ ኣሎ።
|
1.234089
|
Mwina mumpingo wanu muli m'bale amene zochita kapena zolankhula zake sizimakusangalatsani.
|
ምናልባት ብዘረባኡን ብተግባራቱን ቅጭ ዜምጽኣልካ ሓው ኣብ ጉባኤኻ ይህሉ ይኸውን።
|
1.233455
|
Komano zikugwirizana bwanji ndi nkhani yokhudza Ufumu wa Mulungu komanso chaka cha 1914?
|
ግናኸ እዚ ምስ መንግስቲ ኣምላኽ ኰነ ምስ 1914 እንታይ ርክብ ኣለዎ፧
|
1.233444
|
14 Makolo achikhristu amafunikanso kulimba mtima.
|
14 ክርስትያን ወለዲ እውን ትብዓት የድልዮም እዩ።
|
1.233287
|
Yesu ananenanso kuti: "Ndili ndi zambiri zakuti ndikuuzeni, koma padakali pano simungathe kuzimvetsa zonsezo."
|
የሱስ ቀጺሉ፡ "ገና ብዙሕ ዝነግረኩም ኣሎኒ፣ ግናኸ፡ ሕጂ ኽትጾርዎ ኣይትኽእሉን ኢኹም" በሎም።
|
1.232467
|
Popeza Mulungu ndi wamuyaya, zaka 1,000 zili ngati tsiku limodzi kwa iye.
|
ኣምላኽ ዘለኣለማዊ ስለ ዝዀነ፡ ሽሕ ዓመት ንዕኡ ልክዕ ከም ሓንቲ መዓልቲ እዩ።
|
1.232137
|
(ndikuyamba) m'dzina la Allah, kuyamikidwa konse ndi kwa Allah.
|
ብስም ኣላህ እቲ ፍጹም ርህሩህ እቲ ኣዝዩ ራህራሂ
|
1.232039
|
Ngati mutaganizira zimene Mulungu wachitira anthu onse komanso inuyo panokha, n'zoonekeratu kuti watichitira zinthu zambirimbiri.
|
ብዛዕባ እቲ ኣምላኽ ንዓኻን ንደቂ ሰብ ብሓፈሻን ዝገበረልኩም ነገራት ምስ እትሓስበሉ፡ ዛጊት ብዙሕ ነገራት ከም ዝገበረ ንጹር እዩ።
|
1.231929
|
Bambo anga okha ndi amene anabwerako ndi moyo.
|
ኣቦይ ጥራይ ከኣ እዩ ብህይወት ተሪፉ።
|
1.231765
|
Iye anati: "Ndikupatsani inu lamulo latsopano, kuti mukondane wina ndi mnzake; monga ndakonda inu, kuti inunso mukondane wina ndi mnzake.
|
ኣስዕብ ኣቢሉ ኸኣ፡ "ንሓድሕድኩም ክትፋቐሩ፡ ከምቲ ኣነ ዘፍቀርኩኹም፡ ንስኻትኩም እውን ንሓድሕድኩም ክትፋቐሩ፡ ሓድሽ ትእዛዝ እህበኩም ኣለኹ።
|
1.231663
|
Iwo ali nawo maso koma iwo sakukhoza kupenya.
|
ኣዒንቲ ኣለዎም፡ ግናኸ ኣይርእዩን፣
|
1.231573
|
Ndimasangalala kwambiri kukhala mu utumiki tsiku lonse limodzi ndi mkazi wanga."
|
ምስ ሰበይተይ ምሉእ መዓልቲ ኣብ ኣገልግሎት ከሕልፎ ኸለኹ፡ ብሓቂ ዜሐጕስ እዩ" በለ።
|
1.23109
|
5 Tamverani abale anga okondedwa.
|
5 ፍቑራት ኣሕዋተየ ስምዑ።
|
1.230631
|
Mayi wina dzina lake Gail, yemwe panopa ali ndi zaka 60, anati: "Mwamuna wanga Robert, anamwalira pa 9 July, mu 2008, atachita ngozi.
|
"ብዓል ቤተይ ሮበርት ኣብ 9 ሓምለ 2008 እዩ ሞይቱ።
|
1.229993
|
Ngakhale akuchimwire maulendo 7 pa tsiku, n'kubwera kwa iwe maulendo 7, kudzanena kuti, 'Ndalapa ine,' umukhululukire ndithu."
|
ኣብ መዓልቲ ሸውዓተ ሳዕ እኳ እንተ በደለካ፡ 'ተጣዒሰ' እናበለ ኸኣ ሸውዓተ ሳዕ ናባኻ እንተ ተመሊሱ፡ ሕደገሉ።
|
1.229601
|
Iye ananena kuti atumwi okhulupirikawo limodzi ndi anthu ena adzalamulira ndi Yesu kumwamba.
|
እወ፡ እቶም እሙናት ሃዋርያትን ካልኦትን ኣብ ሰማይ ምስኡ ሓቢሮም ኪገዝኡ እዮም።
|
1.229484
|
Ndithudi Allah akudziwa, pomwe inu simudziwa (chinsinsi cha zinthu.)
|
እና ፈለጥኩም ዘይከውን ኣይትስርሑ።
|
1.229214
|
"Allah amafafaniza zimene wafuna ndi kulimbikitsa (kuti zisachoke zomwe wafuna), ndipo gwero la malamulo onse lili kwa Iye (Allah).
|
እቲ ጸጊሙ ዘሎ ሰብ ቦታ አምላኽ ሒዙ በቲ ንሱ ዝደልዮ ንኸምኡ ዝበለ ሰብ ክመርሕ ምድላዩ እዩ።
|
1.228941
|
Anthu ena ali ngati Nowa.
|
ገሊኦም ሰባት ከም ኖህ እዮም።
|
1.228871
|
Mawu ake anali akuti: 'Mphunzitsi wanu ndi mmodzi yekha, [Khristu] ndipo nonsenu ndinu abale.'
|
ይ ዝተወስደት 'ጐይታኹም ሓደ ጥራሕ እዩ ንስኹም ኩሉኹም ኣሕዋት ኢኹም' እትብል እያ።
|
1.228679
|
Kodi ndimafuna nditakhala munthu wamakhalidwe otani? - Akolose 3:10.
|
እንታይ ዓይነት ሰብ እየ ክኸውን ዝደሊ፧ - ቈሎሴ 3:10።
|
1.228636
|
Ngakhale babanga asadziwa pyenepi.'
|
ኣቦይ እውን ነዚ ይፈልጦ እዩ' በሎ።
|
1.228214
|
8 "Kudzachitika zivomezi zamphamvu."
|
8 'ብርቱዕ ምንቅጥቃጥ ምድሪ ኪኸውን እዩ።
|
1.228123
|
1Pe 5:6 Potero dzichepetseni pansi pa dzanja la mphamvu la Mulungu, kuti panthawi yake akakukwezeni:
|
6 ደጊም ብጊዜኡ ንሱ ልዕል ምእንቲ ኼብለኩም፡ ኣብ ትሕቲ እታ ጽንዕቲ ኢድ ኣምላኽ ትሕት በሉ።
|
1.228025
|
64 Koma pali ena mwa inu amene sakhulupilira.
|
64 ገለ ኻባኻትኩም ግና ዘይኣምኑ ኣለዉ" በሎም።
|
1.227925
|
Anthu amenewa amaona kuti safunikira Mulungu pa moyo wawo.
|
እዞም ሰባት እዚኦም፡ ኣምላኽ ከም ዘየድልዮም ኰይኑ እዩ ዚስምዖም።
|
1.227893
|
Kapena atamupempha nsomba, kodi angamupatse njoka?
|
ወይ ከዓ ዓሳ እንተለመኖ ተመን ዝህቦ?
|
1.227666
|
4 Satana sanalenge chinthu ngakhale chimodzi.
|
4 ሰይጣን ዋላ ሓንቲ ኣይፈጠረን።
|
1.227023
|
Pamenepo anawatseguliratu maganizo awo kuti amvetse tanthauzo la Malemba."
|
"ነቲ ቕዱሳት ጽሑፋት ኬስተውዕልዎ፡ ኣእምሮኦም ከፈተሎም።
|
1.226542
|
"Ndipo akadafuna Allah akadawachita iwo kukhala mpingo umodzi; koma amamulowetsa ku chifundo Chake amene wamfuna ndipo odzichitira okha chinyengo (pokana Allah) alibe mtetezi kapena mthandizi.
|
ኢሳይያስ ንዝደለዮ ይኽዕቦ፡ ንዝደለዮ ይኣስሮ ይቀትሎ፡ ንዝደልዮ ይሰጎ፡ ንዝደልዮ ይሸሞ።
|
1.226538
|
Sindinkadziwa chilichonse chokhudza Mulungu woona.
|
ብዛዕባ እቲ ናይ ሓቂ ኣምላኽ ዋላ ሓንቲ ኣይፈልጥን እየ ነይረ።
|
1.226481
|
11 Pakuti Mwana wa Munthu adadza kudzapulumutsa chotayikacho.
|
11 ወዲ ሰብ ንዝጠፍኤ ኼድሕን መጺኡ ኣሎ እሞ፡
|
1.226377
|
Lilime lili ndi mphamvu pa imfa ndi moyo; wolikonda adzadya zipatso zake.
|
ሞትን ህይወትን ኣብ ስልጣን መልሓስ እዩ፡ እቲ ዜፍቅራ ኸኣ ፍሬኣ ኺበልዕ እዩ።
|
1.226273
|
"Ndipo monga masiku a [Nowa] kotero kudzakhala kufika kwake kwa mwana wa munthu.
|
ከምዚ ድማ በለ፦ "ከምቲ ብዘመን ኖህ ዝዀነ፡ ወዲ ሰብ ኣብዚ ኣብ ዚህልወሉ እዋን [ወይ፡ ዳሕሮት መዓልትታት] ከኣ ከምኡ ኪኸውን እዩ።
|
1.225899
|
Ndiyeno akuti kwa ophunzira ake: "Tiyeni tipitenso ku Yudeya."
|
7 - ድሕርዚ ንደቀ መዛሙርቱ፡ ደጊም ንዑናይ፡ ናብ ምድሪ ይሁዳ ንኺድ፡ በሎም።
|
1.225323
|
"Ameneyu adzakhala wamkulu nadzatchedwa Mwana wa Wam'mwambamwamba.
|
ንሱ ዓብዪ ኪኸውን፡ ወዲ እቲ ልዑል እውን ኪብሃል እዩ፣ .
|
1.224535
|
"Sindidalenge ziwanda {Majini} ndi anthu koma kuti azindipembedza."
|
"ጋኔንንና (አጋንንት) ሰብን ክግዙ እለይ እምበር ንካልእ አይፈጠርኩዎምን"
|
1.224382
|
Zolakalaka za anthu oyipa sizidzachitika konse.
|
ת [ታው] ትምኒት እኩያት ኪጠፍእ እዩ።
|
1.223812
|
5Farao anati kwa Yosefe, "Abambo ako ndi abale ako abwera kwa iwe.
|
5 ፈርኦን ድማ ንዮሴፍ፤ ኣቦኻን ኣሕዋትካን መጺኦምኻ።
|
1.22307
|
Iwo anafika ponena kuti: "Ife ndife mboni za zinthu zonse zimene anachita."
|
ብዝኾነ "ተግባር ኢዩ ምስክር" ኢልና ተበጊስና።
|
1.222839
|
Komabe, m'kupita kwa nthawi Solomo anakwatira akazi achilendo ambirimbiri.
|
ሰሎሞን ግና ካብ ካልኦት ሃገራት ብዙሓት ኣንስቲ ተመርዓወ።
|
1.222838
|
"Ngakhale kuti simunamuonepo, mumamukonda.
|
"ንዕኡ ኸቶ እኳ እንተ ዘይረኣኹምዎ፡ ተፍቅርዎ ኢኹም።
|
1.222576
|
64 Koma pali ena mwa inu amene sakukhulupirira."
|
Tigr 64ግና ካባኻትኩም ገሊኣቶም ዘይኣምኑ ኣለዉ፤ በሎም።
|
1.222463
|
2 Nawonso angelo ndi alaliki.
|
2 መላእኽቲ እውን ወንጌላውያን እዮም።
|
1.22208
|
Mwenzi utamvera malamulo anga mtendere wako ukanakhala ngati mtsinje, ndi chilungamo chako monga mafunde a nyanja."
|
ኣየ: ትእዛዛተይ ሰሚዕካ እንተ ትኸውንሲ: ሰላምካ ኸም ወሓዚ: ጽድቅኻውን ከም ማዕበል ባሕሪ ምዀነ ነይሩ።
|
1.221827
|
Iwo anafika mpaka pokana Mwana wa Mulungu.
|
ሕሉፍ ሓሊፎም ንወዲ ኣምላኽ እውን ኣይተቐበልዎን!
|
1.221403
|
Limati: "Kunena za tsikulo kapena ola lake, palibe amene akudziwa, ngakhale angelo kumwamba kapenanso Mwana, koma Atate okha.
|
ከምዚ ዚብል ነንብብ፦ "ብዛዕባ እታ መዓልቲ እቲኣ ወይ እታ ሰዓት እቲኣ፡ ኣቦ እምበር፡ መላእኽቲ ሰማይ ኰኑ ወይስ ወዲ ዀነ፡ ሓደ እኳ ዚፈልጥ የልቦን።
|
1.221374
|
11 Mbwenye, Abheli acita cinthu cakufunika kakamwe.
|
11 ይኹን እምበር፡ ኣቤል ዝያዳ ኣገዳሲ ዝዀነ ነገር ገይሩ እዩ።
|
1.221181
|
Mulungu analenga anthu awiri, Adamu ndi Hava, ndipo anawauza kuti: "Muberekane, muchuluke, mudzaze dziko lapansi."
|
ኣምላኽ ንኽልተ ሰባት፡ ማለት ንኣዳምን ንሄዋንን ፈጠሮም እሞ፡ "ፍረዩን ተባዝሑን ንምድሪ ኸኣ ምልእዋን ምለኽዋን" በሎም።
|
1.220932
|
Mudandipasa wanthu anitsogolela munjila yachadidi, nakulungama.
|
መገዱን ቅንዕንኡን ኣርእዩና።
|
1.220905
|
16 Mariya ankamvetsera kwambiri anthu ena akamalankhula.
|
16 ማርያም ብኸመይ ከም ዝሰምዐት።
|
1.220598
|
Kodi bwanji sathokoza (Allah)?
|
ኣግኣዚያን ይዕወትዶ ኣይዕወትን?
|
1.22016
|
Ndithudi Allah akudziwa, pomwe inu simudziwa (chinsinsi cha zinthu.)
|
ንዘይትፈልጦም አማልኽቲ ድማ ትሰግደሎም።
|
1.219655
|
Kodi kapolo wokhulupirika adzalandira mphoto yaikulu kumwamba kuposa odzozedwa ena?
|
እቲ እሙን ባርያ ኣብ ሰማይ ካብቶም ካልኦት ቅቡኣት ዝዓበየ ዓስቢ ድዩ ዚቕበል፧ ግለጽ።
|
1.219649
|
Umboni wawo ulembedwa ndipo adzafunsidwa (pazimenezo)!
|
ንብቕዓቶም እውን ኣብ ሕቶ የእትውዎ ይዀኑ።
|
1.219597
|
Tsiku lililonse kumabwera anzanga kudzacheza nane.
|
ነፍሲ ወከፍ መዓልቲ፡ ፈተውተይ ኪበጽሑኒ ይመጹ እዮም።
|
1.219488
|
Zitatero anthuwo anati: 'Zonse zimene Yehova wanena tidzachita zomwezo ndipo tidzamumvera.'
|
ንሳቶም ከኣ፡ እግዚኣብሄር ዝበሎ ዅሉ ንገብር፡ ንእዘዝ ድማ፡ በሉ።
|
1.219323
|
Ndithudi Allah akudziwa, pomwe inu simudziwa (chinsinsi cha zinthu.)
|
እትፈልጦ እንተ ዘይብልካ (ዘይኰውን እኳ እንተ መሰለ) ፡ ገለ ነገር ኣይትጥቀስ።
|
1.219216
|
"Anthu anu adzadzipereka eni ake"
|
"ህዝብኻ ፈትዩ ይመጽእ"
|
1.219032
|
Mulungu anakupulumusa iwe pabodzi na anthu onsene."
|
ንሱ ኸኣ መልኣኽ ኣብ ቤቱ ደው ኢሉ፥ 'ንኢዮጴ ልኣኽ እሞ ነቲ ጴጥሮስ ዚብሃል ስምዖን ጸዊዕካ ኣምጽኣዮ፥ ንስኻን ኵሉ ቤትካን እትድኅኑሉ ቓል ንሱ ኪነግረካ እዩ፥' ኪብሎ ኸሎ ከም ዝረኣየ ነገረና።
|
1.218697
|
Muzifunafuna Ufumu Osati Zinthu Zina
|
ስጋዊ ነገራት ዘይኰነስ፡ መንግስቲ ኣምላኽ ድለ
|
1.218682
|
10Ndimakufunafunani ndi mtima wanga wonse;
|
10በሙሉ ልቤ ፈለግሁህ፤
|
1.218605
|
Ndipo Mulungu adzapukuta misozi yonse m'maso mwawo."
|
ኣምላኽ እውን ካብ ኣዒንቶም ንብዓት ዘበለ ኺደርዝ እዩ" ትብል።
|
1.218464
|
Choncho mdzadziwa mmene lilili chenjezo Langa (pa inu).
|
ማሕፉዳይ ርእዩ ፡ መዝገበይ ኣጽኒዑ
|
1.218343
|
Mulungu ndi nkulu kupiringana mitima yathu (19-24)
|
ኣምላኽ ካብ ልብና ይዓቢ (19-24)
|
1.218285
|
Koma akabwera, mzimu wa chowonadi, adzakutsogolelani m'choonadi chonse, pakuti sadzalankhula zake zokha, koma zomwe adzamva adzalankhula, nanena kwa inu za zinthu zomwe zikubwera. "
|
እቲ መንፈስ ሓቂ ምስ መጸ ግና ናብ ኩሉ ሓቂ ዘበለ ኺመርሓኩም፤ ንሱ ነቲ ዝሰምዖ ዘበለ እዩ ዚዛረብ እምበር ካብ ርእሱ ኣይዛረብን እዩ።
|
1.218183
|
Iye wakuyendayo mokwanira, nachita chilungamo, nanena zoonadi mu mtima mwake."
|
እቲ ብቕንዕና ዚመላለስን ጽድቂ ዚገብርን ብልቡ ሓቂ ዚዛረብን።
|
1.218062
|
Koma ngati palibe, udzabwerera kwa inu."
|
እንተ ዘየልቦ ግና፡ ሰላምኩም ኪምለሰኩም እዩ" በሎም።
|
Chichewa-Tigrinya_Sentence-Pairs Dataset
This dataset contains sentence pairs for African languages along with similarity scores. It can be used for machine translation, sentence alignment, or other natural language processing tasks.
This dataset is based on the NLLBv1 dataset, published on OPUS under an open-source initiative led by META. You can find more information here: OPUS - NLLB-v1
Metadata
- File Name: Chichewa-Tigrinya_Sentence-Pairs
- Number of Rows: 196856
- Number of Columns: 3
- Columns: score, Chichewa, Tigrinya
Dataset Description
The dataset contains sentence pairs in African languages with an associated similarity score. Each row consists of three columns:
score: The similarity score between the two sentences (range from 0 to 1).Chichewa: The first sentence in the pair (language 1).Tigrinya: The second sentence in the pair (language 2).
This dataset is intended for use in training and evaluating machine learning models for tasks like translation, sentence similarity, and cross-lingual transfer learning.
References
Below are papers related to how the data was collected and used in various multilingual and cross-lingual applications:
[1] Holger Schwenk and Matthijs Douze, Learning Joint Multilingual Sentence Representations with Neural Machine Translation, ACL workshop on Representation Learning for NLP, 2017
[2] Holger Schwenk and Xian Li, A Corpus for Multilingual Document Classification in Eight Languages, LREC, pages 3548-3551, 2018.
[3] Holger Schwenk, Filtering and Mining Parallel Data in a Joint Multilingual Space ACL, July 2018
[4] Alexis Conneau, Guillaume Lample, Ruty Rinott, Adina Williams, Samuel R. Bowman, Holger Schwenk and Veselin Stoyanov, XNLI: Cross-lingual Sentence Understanding through Inference, EMNLP, 2018.
[5] Mikel Artetxe and Holger Schwenk, Margin-based Parallel Corpus Mining with Multilingual Sentence Embeddings arXiv, Nov 3 2018.
[6] Mikel Artetxe and Holger Schwenk, Massively Multilingual Sentence Embeddings for Zero-Shot Cross-Lingual Transfer and Beyond arXiv, Dec 26 2018.
[7] Holger Schwenk, Vishrav Chaudhary, Shuo Sun, Hongyu Gong and Paco Guzman, WikiMatrix: Mining 135M Parallel Sentences in 1620 Language Pairs from Wikipedia arXiv, July 11 2019.
[8] Holger Schwenk, Guillaume Wenzek, Sergey Edunov, Edouard Grave and Armand Joulin CCMatrix: Mining Billions of High-Quality Parallel Sentences on the WEB
[9] Paul-Ambroise Duquenne, Hongyu Gong, Holger Schwenk, Multimodal and Multilingual Embeddings for Large-Scale Speech Mining, NeurIPS 2021, pages 15748-15761.
[10] Kevin Heffernan, Onur Celebi, and Holger Schwenk, Bitext Mining Using Distilled Sentence Representations for Low-Resource Languages
- Downloads last month
- 17