score
float32
1.04
1.25
Chichewa
stringlengths
10
491
Umbundu
stringlengths
10
498
1.249944
"Mudzakhala Mboni Zanga"
"Vu Linga Olombangi Viange"
1.249851
Choncho anaitana mmodzi wa antchito ndi kumufunsa chimene chinali kuchitika.
Kuenje wa vilikiya umue pokati kapika yu wo pula eci ca kala oku pita.
1.249559
Titeteze Mitima Yathu 37.
Tu Lavi Utima Wetu 37.
1.249531
May 2015 _ Kodi Mapeto Ali Pafupidi?
Kupemba 2015 _ Esulilo li Kasi hẽ Ocipepi?
1.249459
Kodi n'chiyani chikanathandiza Aisiraeli kudziwa kuti Mose anali ndi mzimu wa Mulungu?
Ovaisrael ova li tava dulu okudidilika mo ngahelipi kutya Moses okwa li e na omhepo yaKalunga?
1.249406
Nsiku iri-yense imbakwane na bzakuipa bzace.'
Ohali yeteke liongongo yi tẽla eteke liaco.'
1.249366
"Mwasambitsidwa kukhala oyera, mwapatulidwa." - 1 AKOR.
'Wa sukuiwi, kuenda wa yelisiwi.' - 1 VA KOR.
1.2493
"Ndipo monga masiku a [Nowa] kotero kudzakhala kufika kwake kwa mwana wa munthu.
Eye wa popia ndoco: "Ndeci ca kala koloneke via Noha, haico ci kala ketukuluko lia Mõlomunu [ale koloneke via sulako].
1.249202
December 2014 _ Mulungu Akhoza Kukhala Mnzanu Wapamtima
Cembanima 2014 _ O Pondola Oku Kuata Ukamba la Suku
1.249
Pamene ine ndili m'dziko, ndine kuwala kwa dzikoli."
Osimbu ndi kasi voluali, ndicinyi coluali."
1.248972
Atate inu, musakwiyitse ana anu, kuti angataye mtima.
Ene alonjali, ko ka wenguli onyeño yomãla vene, sanga va konyõha.'
1.248925
Ndikuona kuti tsopano ndine munthu wosangalala kusiyana ndi kale." - A Karen.
Cilo ñuete esanju lia lua." - Karen.
1.248907
'Muyeruzi wa Dziko Lense' Ambacita Bzinthu Mwacirungamo Nthawe Zense
"Onganji Yoluali Luosi" Olonjanja Viosi yi Linga Ovina Via Sunguluka
1.248839
Zoipa za tsiku lililonse n'zokwanira pa tsikulo.'
Ohali yeteke liongongo yi tẽla eteke liaco.'
1.248819
Pafupifupi 500 mwa iwo ndi alongo osakwatiwa.
Pokati kavo pakala eci cisoka 500, vamanji akãi okuti ka va kuelele.
1.248406
Sali Mulungu wa akufa, koma wa amoyo: musocera inu ndithu.
Eye ha Sukuko yava va fa, te yava va kasi lomuenyo.
1.248298
Ndidzamuteteza chifukwa wadziwa dzina langa."
Ndu u teyuila omo a kũlĩha onduko yange.'
1.24829
Munthu amene akuyenda alibe ulamulilo wowongolela mapazi ake."
" Omunu enda ka tẽla eye muẽle oku suñamisa oku enda kuaye. "
1.247864
'Apanga Zinthu Zonse Kukhala Zatsopano' 147.
'Ovina Viosi vi Linga Viokaliye' 147.
1.247729
Buluka penepo akhabwerera ku nzinda wace wa Rama.
Noke wa tiukila kimbo liaye ko Rama.
1.247716
Siali a dziko lapansi monga Ine sindili wa dziko lapansi."
Ovo havakualualiko ndeci ame siukualualiko."
1.247655
Mungathe Kukhala Bwenzi la Mulungu!
Citava Okuti Okala Ekamba lia Suku!
1.247562
N'chifukwa Chiyani Timakalamba Komanso Kumwalira?
Momo lie tu kukila kuenda tu fila?
1.24736
Mayi awo a mayi angawa anaphunzira choonadi mu 1908.
Ina yange wa lilongisa ocili Cembimbiliya kunyamo wo 1908.
1.247193
Pamenepo ophunzirawo anati: 'Ambuye, ngati iye akupumula, apeza bwino.'
Kuenje olondonge viaye vi popia viti: "A Ñala, nda wa pekela, o kala ciwa."
1.247178
Ineyo ndinkadzitenga kuti ndine Msilamu.
Ame nda litendele ndu okuti nda tiamẽla ketavo lia va Musulumanu.
1.247166
'Ndimbafunadi lamulo lanu!
"Sole cimue ovihandeleko viove.
1.247118
Pamenepo anawatseguliratu maganizo awo kuti amvetse tanthauzo la Malemba."
Eye, "wa situlula ovitima viavo okuti va limbuka ovisonehua."
1.247068
Pa nthawiyi, n'kuti dziko la Hungary lili pansi pa ulamuliro wachikomyunizimu.
Kotembo yaco, ofeka yo Hungria ya kala vemehi liuviali wo komunismo.
1.247021
Ndisaunyerezera ntsiku yonsene." - Masal.
Ndukuaku vi sokolola ño-o eteke liosi." - Osa.
1.246995
ndipo Iye sanalole aliyense kugulitsa malonda mʼmabwalo a Nyumba ya Mulungu.
Ova li hava hongo ovanhu pandjikilile motembeli.
1.246993
Iye anati: "Atate, ngati mukufuna, ndicotseleni kapu iyi.
Eye wa popia hati: "A Tate, nda wa panga, njupe okopo eyi.
1.246912
Kodi N'chifukwa Chiyani Timakalamba Komanso Kufa?
Momo lie tu kukila kuenda tu fila?
1.246898
Iye anati: "Mulungu amene ayankhe potumiza moto ndiye Mulungu woona."
Okwa ti kutya "Kalunga ou ta nyamukula nomundilo, Oye Kalunga."
1.246861
Osasandutsa Nyumba ya Atate anga msika!"
Ko ka lingi onjo ya Isiange ocitumãlo cimue colomĩlu!'
1.246821
"Ine ndine mkate wamoyo.
"Ame ndimbolo yomuenyo.
1.246704
Motero sazindikira zimene dzuŵa limatiphunzitsa.
Ovo vasiapo oku limbuka eci ekumbi li pondola oku tu longisa.
1.246691
Komano zikugwirizana bwanji ndi nkhani yokhudza Ufumu wa Mulungu komanso chaka cha 1914?
Pole, ovina viaco vi tiamisiwila ndati Kusoma wa Suku kuenda kunyamo wo 1914?
1.246654
"Ndinali Ndisanapatsidwepo Mphatso Yamtengo Wapatali Ngati Imeneyi"
"Eyi Oyo Ombanjaile ya Velapo Nda Tambuile"
1.24606
Mu 2008, Paolo anauzidwa kuti ali ndi matenda a khansa.
Kunyamo wo 2008, ulume wange Paolo wa limbuka okuti, o kuete uvei wo kanser.
1.246023
Komano n'chifukwa chiyani tiyenera kusankha kukonda Mulungu?
Momo lie tu nõlelapo oku sola Suku?
1.245974
Koma ena amene poyamba anali olambila mafano anaona kuti kudya nyamayo ni kulambila fano.
Ashike vamwe ovo va li hava longele nale oikalunga ova li ve udite kutya okulya ombelela oyo okuli onghedi yokulongela oikalunga.
1.245916
Uzim'kumbukira m'njira zako zonse, ndipo iye adzawongola njira zako." - Miy.
Sumbila Suku kovina viosi o linga, kuenje eye o suñamisa olonjila viove.' - Olosap.
1.245872
Pabodzi na Janet pa ntsuwa ibodzi ya ku Filipina
Lukãi wange Janet, eci tua kala kocifuka cimue kofeka yo Filipina
1.245865
"Ngati ndi kotheka, khalani mwamtendere ndi anthu onse, monga mmene mungathere.
"Nda citava, kali vakuambembua lomanu vosi.
1.24581
Kapena ndani anakupatsani ulamuliro umenewu?" - Maliko 11:28.
Kuenda wa ku ĩha omoko yoku linga ovina evi elie?" - Marko 11:28.
1.245736
Kodi ndani adzathetse mavuto a anthu?
Helie o ka tetulula ovitangi viomanu?
1.245684
Taganizirani chitsanzo cha banja lina la ku Asia.
Kũlĩhisa ulandu wohueli yimue okuti, Akristão ko Asia.
1.24568
Chimene chili kwa Allah, ndicho chabwino kwa inu ngati mukudziwa.
Ndomo o kuatisiwa: Suku oku likuminya omuenyo ko pui, nda wa sanda oku u kũliha.
1.245669
Tamandani Ya, anthu inu!"
Vandu " ya.
1.245612
Anthu ena amene tinaphunzira nawo Baibulo
Vamue tua longisa Embimbiliya
1.245541
"Tate wa Onse Okhala ndi Chikhulupiriro"
'Isia ya Vosi va Kuete Ekolelo'
1.245437
Kondwa pabodzi na ine mbuya wako.'
Sanjukila kumue la cime cove.'
1.245384
Tifunika kuulula macimo athu kwa iye.
Otu na okuhepaulula omatimba etu kuye.
1.24528
15 Anthufe nthawi zina sitileza mtima ndi anthu amene timawakonda.
15 Olonjanja vimue ka tu lekisa epandi komanu vana tu kuetele ocisola.
1.245162
Kodi Kupemphera Kungakuthandizeni Bwanji?
Ohutililo - Ndomo yi Pondola Oku ku Kuatisa
1.245115
Kodi pemphero ndi lofunika bwanji kuti ndipulumuke?'
Esilivilo lipi olohutililo vi kuete koku popeliwa kuange?'
1.245105
Koma kodi mukudziwa kuti timaphunziranso Baibulo ndi anthu padziko lonse?
Pole, ove wa kũlĩhavo okuti etu tu kuete esokiyo lioku longisa omanu Embimbiliya koluali luosi?
1.245088
"Tipatseni Chakudya chathu
"Tu ĩhe okulia kuetu kuetaili."
1.245033
Tilimbikitsane Wina na Mnzake 91.
Tu Livetiyi Pokati 91.
1.244976
Mukhoza Kudzakhala Padzikoli Kwamuyaya
O Pondola Oku Kala Otembo ka yi Pui Palo Posi
1.244775
Iwo akhafuna kudziwa kuti mbani akhali wakufunika kakamwe pakati pawo.
Va enda oku lihoyisa catiamẽla komunu wa velapo pokati kavo.
1.244772
Ambiri amada nkhawa akaganizira zam'tsogolo ndipo alibe chiyembekezo.
Valua pokati kavo va sakalala lovina vi keya kovaso yoloneke, kuenda ka va kuete elavoko.
1.244761
Kodi anthufe tinachokera ku nyama?
Etu hẽ tua tunda kovinyama?
1.244649
Sathani alonga: 'Mulungu asadziwa kuti, ntsiku inadzadya imwe, maso anu anadzafunguka.'
Satana wa popia hati: "Suku wa kulĩha okuti eteke vu liako, ovaso ene haico a letuluka."
1.244648
Ndidzamuteteza chifukwa wadziwa dzina langa." - SAL.
Ndu u teyuila omo a kũlĩha onduko yange.' - OSA.
1.244553
Pamenepo anawatseguliratu maganizo awo kuti amvetse tanthauzo la Malemba."
Ombibeli oya ti: "Okwe va fatululila eendunge davo okushiiva omishangwa."
1.244542
Mwamuna ananena kuti: "Titangokwatirana kumene, ine ndi mkazi wanga tinali ndi maganizo osiyana pa nkhani ya mmene tingamasonyezerane ulemu.
Ulume o popia hati: "Eci tua kuela, ame lukãi wange ka tua kuatele ocisimĩlo cimuamue catiamẽla kesumbilo.
1.244523
"Anthuwo sadzaphunziranso nkhondo"
"Ndaño ovita ka va vi lilongisa vali"
1.2445
Mu caka 1937, dzina yadzacinjwa mbikhala Consolação.
Kunyamo wo 1937, onduko yaco ya pongoluiwa okuti, Consolação.
1.244491
"Woweluza wa Dziko Lonse" Amacita Cilungamo Nthawi Zonse
"Onganji Yoluali Luosi" Olonjanja Viosi yi Linga Ovina Via Sunguluka
1.244428
Leka 'Kufunafuna Zinthu Zazikulu'
Ku ka 'Lisandele Ovina Vinene'
1.244337
Munthu akafa, ndiye kuti wapereka malipiro a machimo ake okha basi.
Eci tu fa, tu feta onima yi tunda kekandu lietu muẽle.
1.244191
Ndimasinkhasinkha chilamulocho tsiku lonse.
Ndukuaku vi sokolola ño-o eteke liosi.
1.244138
Marita anayankha mwachidaliro kuti: "Ndidziwa kuti adzauka m'kuuka tsiku lomaliza."
Marta wa popia hati: 'Nda kolela okuti eye o ka pinduka kepinduko lia sulako.'
1.244029
Ndiponso, ndiye Atate amene tonsefe timafunikira.
Handi vali, Eye eye Isia tu sukila vosi yetu.
1.243975
"Munthu amene akuyenda alibe ulamuliro wowongolera mapazi ake."
" Omunu enda ka tẽla eye muẽle oku suñamisa oku enda kuaye. "
1.243932
(Genesis 41:45) Kodi atamuona anazindikira kuti ndi Yosefe?
(Efetikilo 41:45) Eci ovo vo mola, va limbuka hẽ okuti eye Yosefe?
1.243917
12 Ine ndisapimana ca kudya kawiri pa sumana, pontho pa pinthu pyanga pyonsene pina wina ine, ndisabulusa ca cikhumi."
Ndi likandangaya okulia luvali kosimanu, ndukuakulumba onepa yekui yovipako viange viosi."
1.243893
May 2014 _ Kodi Pali Amene Angadziwiretu za M'tsogolo?
Kupemba 2014 _ Omunu hẽ o pondola oku kũlĩha eci ci keya kovaso yoloneke?
1.243739
Kodi ndani angathetsedi umphawi?
Helie o pondola oku malako uhukũi?
1.243569
Napo wanthu acititsutsa,
Momo wosi ka tamalala letu, o kasi letu.
1.243529
Izi n'zimene Mfumu Davide anachita.
Eci oco ca linga Soma Daviti.
1.243333
Atumiki anga adzamwa, koma inuyo mudzakhala ndi ludzu.
Tala, akuenje vange va nyua, ene puãi vu kala lenyona.
1.242682
Mukatero mtendere wanu udzakhala ngati mtsinje, ndipo chilungamo chanu chidzakhala ngati mafunde a m'nyanja."
Nda ombembua yove nda ya lingile ndolui, kuenda esunga liove ndapuku okalunga."
1.242676
Kodi Aisiraeli anamvera malangizo ati?
Va Isareli va pokola kolonumbi vipi?
1.242647
N'zoona kuti sitingadziwe zomwe Ahabu anali kuganiza panthawiyo.
Ocili okuti ka tua kũlĩhĩle ovisimĩlo Ahava a kuata kepuluvi liaco.
1.24264
Mayi Phiri: Tsopano ndayamba kumvetsa.
Sophia: Nda limbuka ocisimĩlo cove.
1.242341
Natenepa, iye acemera nyabasa m'bodzi mbasaka kudziwa kuti ninji pikucitika.
Kuenje wa vilikiya umue pokati kapika yu wo pula eci ca kala oku pita.
1.242
Mukanandidziwa Ine, mukanawadziwanso Atate anga."
Nda wa ñũlĩhĩli, nda wa kũlĩhivo Isiange."
1.241992
M'Baibulo muli nkhani zambiri zosonyeza kuti iye amadalitsa atumiki ake okhulupirika.
Vembimbiliya tu sangamo ovolandu a lekisa ndomo Suku a eca onima kafendeli vaye vakuekolelo vo kosimbu.
1.241957
Pomwe Jeremiya adadzaikumbukira bwino-bwino nkhaniyo, iye adati: 'Mafala ya Yahova yankugaka mu mtima mwangumu ninga moto.
Yeremiya poku sokolola catiamẽla kovina viaco, wa popia hati: 'Esapulo lia Yehova li kasi ndondalu yimue vutima wange.
1.24183
Ine na Janet tiri pa ibodzi mwa ntsuwa za ku Filipinas
Lukãi wange Janet, eci tua kala kocifuka cimue kofeka yo Filipina
1.241793
Choncho ndili ndi zaka 18 ndinachoka panyumba.
Eci nda tẽlisa 18 kanyamo nda tunda konjo.
1.24171
Inu amuna, kondani akazi anu ndipo musawapsere mtima.
Ovalumenhu nye, holeni ovakainhu veni, nye inamu va ningila onyanya.
1.241598
Zimene Ndinasankha Ndili Mwana
Onjila nda nõla eci nda kala umalẽhe
1.241582
Mayi Phiri: Ee, ndinaphunzirapo nkhani imeneyi ku Sande Sukulu.
Sophia: Ocili, nda lilongisa ulandu waco Komisa ya Calumingu komẽle.
1.241562
Kodi Mulungu adzawachitira chiyani anthu m'tsogolomu? - Werengani Afilipi 1:9.
Nye Suku a ka lingila omanu kovaso yoloneke? - Tanga Va Filipoi 1:9.
1.241468
Kodi munthu aliyense ali ndi mngelo amene amamuteteza?
O Kuete hẽ Ungelo Umue wa Siata Oku ku Teyuila?
1.241404
7 'Kun'dzakhala na njala.'
7 "Ku kala onjala."