Chichewa
stringlengths 10
500
| sentiment
stringclasses 2
values | __index_level_0__
int64 0
835k
|
|---|---|---|
Kodi umboni umenewu ndi otani umene anthu awa akupereka kukutsutsa Iwe?"
|
Negative
| 0
|
Anthu atatu onsewa anasintha chonchi chifukwa choti ankafuna kutsanzira Khristu.
|
Negative
| 1
|
"Ndipo iye pamodzi ndi makamu ake ankhondo adadzitukumula pa dziko popanda chilungamo ndipo ankaganiza kuti iwo sadzabwelere kwa Ife.
|
Negative
| 2
|
njira yanji akuchotsedwa ku (choonadi)!
|
Positive
| 3
|
"Ndipo opani Moto umene wakonzedwa kwa (anthu) osakhulupirira.
|
Negative
| 4
|
"Tawafunsani nkhani ya mudzi umene udali m'mphepete mwa nyanja; (anthu am'mudziwo) pamene adali kuswa (lamulo la) tsiku la Sabata (lomwe adauzidwa kuti pa tsikuli asamachite usodzi wa nsomba, koma m'malo mwake azichita mapemphero okha).
|
Negative
| 5
|
Amapereka moyo ndikupereka imfa, Mbuye wanu ndi Mbuye wa makolo anu oyamba.
|
Positive
| 6
|
"Ndipo motero tidampatsa ulemelero Yûsuf m'dziko (la Iguputo); amakhala m'menemo paliponse pamene wafuna.
|
Positive
| 7
|
"Ndipo munthu (wokanira) amanena: "Kodi ndikadzafa nzoonadi kuti Ndidzatulutsidwa (m'manda) nkukhala wamoyo?"
|
Negative
| 8
|
Iye anayenda nane mwamtendere ndi molungama mtima, ndipo anabweza anthu ambiri mʼnjira zawo zauchimo.
|
Positive
| 9
|
N'zimene zinawasonkhezera kukwaniritsa zimene anachita."
|
Positive
| 10
|
Kodi Qur'an sinadzudzule ma Arabu achikunja chifukwa
|
Negative
| 11
|
Ngakhale kuti kukhalapo kwake monga Mfumu ya Ufumu wa Mulungu n'kosaoneka, umboni wake ukuoneka chifukwa cha kukwaniritsidwa kwa maulosi.
|
Negative
| 12
|
Ndipo A'adi adaonongedwa ndi chimphepo
|
Positive
| 13
|
Ndipo iye adaitana Mbuye wake kuti: "Awa ndithu ndi anthu oipa."
|
Negative
| 14
|
""Ndithu Allah ndiye Mbuye wanga ndi Mbuye wanunso; choncho mupembedzeni; imeneyi ndiyo njira yolunjika."
|
Positive
| 15
|
"Ndipo kachisanu (alumbire) kuti matembelero a Allah akhale pa iye ngati (iye) ali m'modzi mwa onama.
|
Negative
| 16
|
(Zikadzachitika zimenezi) mzimu Uliwonse udzadziwa zimene Wabweretsa (zabwino ndi zoipa).
|
Positive
| 17
|
Kuti tithawe kuchoka mnyanja yamoto, kulibe njira ina iliyonse koma kuti maina athu alembedwe mu Buku la Moyo.
|
Negative
| 18
|
ndipo amasiyira chuma chawo anthu ena.
|
Positive
| 19
|
"Ndipo ndithu tidasiya chizindikiro mmenemo choonekera kwa anthu anzeru.
|
Positive
| 20
|
Atumize Mzimu Wanu, ndipo iwo adzakhala analenga.
|
Positive
| 21
|
"Kodi saona momwe Allah ayambitsira zolengedwa, kenako nkuzibwerezanso?
|
Negative
| 22
|
"Koma amene waopa kuti adzaimitsidwa kwa Mbuye wake (pa nthawi ya chiweruziro), adzalandira minda iwiri (yaikulu yamtendere).
|
Negative
| 23
|
"Ndipo ngati utawafunsa: "Ndani adawalenga?"
|
Negative
| 24
|
"Ndithu Allah amakonda amene akumenya nkhondo pa njira Yake (yofalitsa chipembedzo Chake), ali pa mzere (umodzi) uku ali monga chomanga, chomangika mwamphamvu.
|
Positive
| 25
|
"M'menemo ndi momwe tikulongosolera mokwanira zivumbulutso kuti mwina iwo angabwelere (kwa Allah).
|
Positive
| 26
|
(Komanso) ndinasonkhanitsa anthu onse (amene ankakhala m'mizindayo) ndipo ndinawalamula kuti abwerere kumizinda yawo."
|
Positive
| 27
|
Ndipo iwo adzakhala ndi moyo m'dziko lawo, limene ndinapatsa mtumiki wanga Yakobo.
|
Positive
| 28
|
Koma amene angafune (zina) Kusiya zimenezi iwowo ndiwo Olumpha malire.
|
Positive
| 29
|
Ndithu m'zimenezo muli malingaliro kwa kapolo aliyense wotembenukira (kwa Allah).
|
Positive
| 30
|
""Ndithu ine ndikukuoperani chilango cha tsiku lalikulu."
|
Negative
| 31
|
Ndipo adzawalowetsa m'minda yomwe pansi pake pakuyenda mitsinje; adzakhala m'menemo muyaya.
|
Positive
| 32
|
" (Zikadzachitika zimenezi) mzimu uliwonse udzadziwa zimene wabweretsa (zabwino ndi zoipa).
|
Positive
| 33
|
Ndithudi, yemwe mudzamulowetse ku Moto ndiye kuti mwamuyalutsa, ndipo sipadzakhala athandizi kwa ochita zoipa."
|
Negative
| 34
|
"Ndipo angelo awiriwa anadza ku Sodomu madzulo, pamene Loti adakhala pachipata cha Sodomu.
|
Negative
| 35
|
Komanso tikulimbikitsidwa ndi mawu akuti: 'Omwe aopa Mulungu adzapeza bwino.'
|
Positive
| 36
|
"Kwa yemwe mwa inu akufuna kuyenda mu njira yoongoka.
|
Positive
| 37
|
Ndipo munthu adati kwa ena,
|
Positive
| 38
|
Ukadzatuluka udzakhala wokalamba komanso wekhawekha."
|
Negative
| 39
|
Qur'an inabvumbulutsidwa Mmwezi wa Ramadhan, choncho Allah anaupanga mwezi wa Ramadhan kukhala wabwino kuposa myezi yonse.
|
Positive
| 40
|
"Ndithu Ife tidawatumizira chimphepo champhamvu choulutsa miyala (ndi kuwagenda), kupatula akubanja la Luti; tidawapulumutsa (ku chilangocho) m'bandakucha,
|
Negative
| 41
|
Thangwe nsiku za wanthu wangu, zin'dzakhala ninga nsiku za muti, ndipo omwe ndawasankhulawo, wan'dzapfatsa na mabasa yakuphatidwa na manja yawo.'
|
Positive
| 42
|
Ndipo opani Allah, dziwani kuti Allah Ngwaukali polanga.
|
Negative
| 43
|
Ine sindili chilichonse koma mchenjezi ndi wouza anthu okhulupirira nkhani zabwino."
|
Positive
| 44
|
Kumwamba kapena kwa anthu?"
|
Positive
| 45
|
Ngati helo alidi malo ozunzirako anthu, m'pake kuopa.
|
Negative
| 46
|
"Kenako kudzanenedwa kwa amene adachita zoipa: "Lawani chilango chamuyaya!
|
Negative
| 47
|
"Ndipo Ayah Zathu zikawerengcdwa kwa iwo zolongosola chilichonse momveka, alibe mtsutso wina koma kunena kuti: "Tibweretsereni makolo Athu (aukitseni akhale ndi moyo) ngati inu muli owona!"
|
Positive
| 48
|
""Kupatula akapolo Anu omwe ali osankhidwa (oyeretsedwa) mwa iwo.
|
Positive
| 49
|
"Nena: "E inu amene mudapatsidwa buku! chifukwa chiyani mukuzikana zizindikiro za Allah pomwe Allah ndi Mboni wa zonse zimene mukuchita?"
|
Negative
| 50
|
Komabe, umboni wosatulutsa mawu wa zinthu zakumwamba ndi wamphamvu kwambiri.
|
Positive
| 51
|
Kotero kodi izo kutsatira kuti ife kuba, ku nyumba ya mbuye wanu, golide kapena siliva?
|
Negative
| 52
|
Ndithu taphunzitsidwa (mpaka tikudziwa) chiyankhulo cha mbalame, ndiponso tapatsidwa chilichonse; ndithu umenewu ndiubwino wopenyeka.
|
Positive
| 53
|
Yosefe atawaona, anazindikira kuti akuda nkhawa ndi zinazake ndipo anawafunsa kuti: "N'chifukwa chiyani nkhope zanu zili zachisoni lero?"
|
Negative
| 54
|
Ndipo ndithu lonjezo lanu ndiloona, ndipo Inu Ndinu Woweruza mwachoonadi kuposa aweruzi onse."
|
Positive
| 55
|
"Ndipo tidampulumutsa iye ndi anthu ake ku vuto lalikulu.
|
Positive
| 56
|
Ngati ndinu wachinyamata ndipo mwakumana ndi zimenezi, muyenera kuganizira za Mose.
|
Negative
| 57
|
Kodi sakuona kuti ilo (fano lawolo) silikuwalankhula ndiponso silikuwaongolera njira (yabwino?)
|
Negative
| 58
|
"Ndithudi, taona kutembenukatembenuka kwa nkhope yako (kuyang'ana) kumwamba.
|
Positive
| 59
|
Ambuye ali pafupi."
|
Positive
| 60
|
Choncho Mulungu anamulanga ndi matenda oopsa akhate.
|
Negative
| 61
|
Ndipo ndithu, lonjezo lanu ndiloona, ndipo inu ndinu Woweruza mwachoonadi kuposa aweruzi onse."
|
Positive
| 62
|
"Onse awa, (abwino ndi oipa), timawapatsa awa ndi awa mwazopatsa za Mbuye wako; ndipo zopatsa za Mbuye wako sizotsekerezedwa (kuti zisamfike kapolo Wake).
|
Positive
| 63
|
Chonchotu, atibweretsere chizizwa monga mmene adatumiziridwa (aneneri) oyamba."
|
Negative
| 64
|
Ameneyu ndiye mwamuwona kuti ndiye wofunika punishment?
|
Negative
| 65
|
Taonani,"Iye anati, "Moto ndi nkhuni.
|
Positive
| 66
|
Kapena kuwadyetsa (osowa) pa masiku a njala.
|
Negative
| 67
|
Kodi angathe kukuthandizani kapena kudzithandiza okha?"
|
Negative
| 68
|
Mbuye wako wanena (kuti): 'Izi nzofewa kwa Ine; ndithu ndidakulenga kale pomwe iwe sudali kanthu."
|
Positive
| 69
|
"Kamuuzeni mawu ofewa mwina akalingalira (uthengawo) kapena akaopa.
|
Positive
| 70
|
"Ndipo (Nuh) adati: "Kwerani m'menemo mwadzina la Allah mkuyenda kwake ndi mkukocheza kwake.
|
Positive
| 71
|
Kapena kuwadyetsa (osowa) pa Masiku a njala
|
Negative
| 72
|
Pamene muwerenga, kumbukirani ndi uthenga wa Mulungu kwa inu ngati munthu.
|
Positive
| 73
|
"Ndipo tidawagawa iwo m'mafuko khumi ndi awiri (osiyanasiyana) monga mitundu ikuluikulu.
|
Negative
| 74
|
mwanayo) adzamuyamwitsira (mkazi) wina,
|
Positive
| 75
|
"Ndipo mwa amene tidawalenga, alipo anthu oongolera (anzawo) ku choonadi.
|
Positive
| 76
|
Kapena angachite mantha kuti zidzawavuta kuchita zimene Mulungu amafuna akadzabatizidwa.
|
Negative
| 77
|
N'chifukwa chiyani wangokhala wekha kupereka ziweruzo ndipo anthu onse ali chiimire pamaso pako kuyambira m'mawa mpaka madzulo?"
|
Negative
| 78
|
Atamuuza vutoli, Yesu anamuuza momveka bwino kuti: "Inu mumalambira chimene simuchidziwa."
|
Positive
| 79
|
Ndiponso sadzawayeretsa (kumachimo awo); ndipo iwo adzapeza chilango chopweteka.
|
Negative
| 80
|
monga mawu omveka, pamene khoma limodzi limaphimbidwa;
|
Negative
| 81
|
Ndithu ine ndikumganizira kuti ndi mmodzi wa abodza."
|
Negative
| 82
|
Mwachitsanzo, Solomo anachonderera Mulungu kuti aziyankha mapembedzero a olambira Ake.
|
Positive
| 83
|
mwa Mulungu ine ndimadaliramo; sindidzachita mantha.
|
Positive
| 84
|
Ndipo, ndithudi, ngati pali mwamuna mu aquarium iyi.
|
Negative
| 85
|
Iwo sayenera amafanana zovala zachimuna kapena zovala za osakhulupirira.
|
Negative
| 86
|
"Pamene m'bale wawo (Mneneri) Hûd adawafunsa kuti: "Kodi simuopa (Allah)?"
|
Positive
| 87
|
"Kufikira pamene adzatidzera (tsiku la Qiyâma, uku akulowetsedwa ku Moto).
|
Positive
| 88
|
Atate, ndipulumutseni Ine ku nthaŵi iyi."
|
Negative
| 89
|
"Mawa lino adzadziwa (tsiku lakuwatsikira chilango,) kuti ndiyani wabodza wodzitukumula (iwo kapena Swaleh).
|
Negative
| 90
|
"Nena: "Yendani pa dziko ndi kuona momwe Allah adayambitsira chilengedwe; kenako Allah adzaumba, kuumba kwina.
|
Positive
| 91
|
Chifukwa ndaona zonse zimene Labani wachita kwa inu.
|
Negative
| 92
|
Amphaka ngati dzina lawo limveka;
|
Positive
| 93
|
"Kotero alemekezeke Yemwe m'manja Mwake muli ulamuliro pa chinthu chilichonse; ndipo kwa Iye (ndiko) mudzabweerera nonse.
|
Positive
| 94
|
"Zimenezo nchifukwa chakuti iwo adakonda moyo wa dziko lapansi kwambiri kuposa wa pambuyo pa imfa; ndi kutinso Allah saongola anthu osakhulupirira.
|
Negative
| 95
|
M'nthaka muli zizindikiro kwa Otsimikiza, (Zosonyeza kuti Mulungu alipo).
|
Positive
| 96
|
ndipo zaka za moyo wako zidzakhala zochuluka.
|
Positive
| 97
|
Uchiteni mzinda uwu (wa Makka) kukhala wa mtendere; ndipo ndipatuleni ine ndi ana anga ku machitidwe opembedza mafano."
|
Positive
| 98
|
Zikomo...izo anali Old School.
|
Positive
| 99
|
Subsets and Splits
No community queries yet
The top public SQL queries from the community will appear here once available.